Pular para o conteúdo
Publicidade

Provérbios 31

24 Iye amasoka nsalu zabafuta nazigulitsa;

amaperekanso mipango kwa anthu amalonda.

25 Mphamvu ndi ulemu zimakhala ngati chovala chake;

ndipo amaseka osaopa zamʼtsogolo.

26 Iye amayankhula mwanzeru,

amaphunzitsa anthu mwachikondi.

27 Iye amayangʼanira makhalidwe a anthu a pa banja lake

ndipo sachita ulesi ndi pangʼono pomwe.

Veja também