Pular para o conteúdo
Publicidade

Provérbios 4

3 Paja ndinalinso mwana mʼnyumba mwa abambo anga;

mwana mmodzi yekha wapamtima pa amayi anga.

4 Ndipo abambo anandiphunzitsa ndi mawu akuti,

"Ugwiritse mawu anga pa mtima pako,

usunge malamulo anga kuti ukhale ndi moyo.

Veja também