3 Paja ndinalinso mwana mʼnyumba mwa abambo anga;
mwana mmodzi yekha wapamtima pa amayi anga.
4 Ndipo abambo anandiphunzitsa ndi mawu akuti,
"Ugwiritse mawu anga pa mtima pako,
usunge malamulo anga kuti ukhale ndi moyo.
3 Paja ndinalinso mwana mʼnyumba mwa abambo anga;
mwana mmodzi yekha wapamtima pa amayi anga.
4 Ndipo abambo anandiphunzitsa ndi mawu akuti,
"Ugwiritse mawu anga pa mtima pako,
usunge malamulo anga kuti ukhale ndi moyo.