Publicidade

Provérbios 4

5 Upeze nzeru, upeze nzeru zomvetsa zinthu;

usayiwale mawu anga kapena kutayana nawo.

6 Usasiye nzeru ndipo idzakusunga.

Uziyikonda ndipo idzakuteteza.

7 Fundo yayikulu pa za nzeru ndi iyi: upeze nzeru.

Kaya pali china chilichonse chimene ungapeze, koma upeze nzeru yomvetsa bwino zinthu.

8 Uyilemekeze nzeruyo ndipo idzakukweza;

ikumbatire nzeruyo ndipo idzakupatsa ulemu.

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-28_14-13-17-