Pular para o conteúdo
Publicidade

MIYAMBO 4

5 Upeze nzeru, upeze nzeru zomvetsa zinthu;

usayiwale mawu anga kapena kutayana nawo.

6 Usasiye nzeru ndipo idzakusunga.

Uziyikonda ndipo idzakuteteza.

7 Fundo yayikulu pa za nzeru ndi iyi: upeze nzeru.

Kaya pali china chilichonse chimene ungapeze, koma upeze nzeru yomvetsa bwino zinthu.

8 Uyilemekeze nzeruyo ndipo idzakukweza;

ikumbatire nzeruyo ndipo idzakupatsa ulemu.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também