Pular para o conteúdo
Publicidade

MIYAMBO 5

3 Pakuti mkazi wachigololo ali ndi mawu okoma ngati uchi.

Zoyankhula zake ndi zosalala ngati mafuta,

4 koma kotsirizira kwake ngowawa ngati ndulu;

ngakuthwa ngati lupanga lakuthwa konsekonse.

5 Mapazi ake amatsikira ku imfa;

akamayenda ndiye kuti akupita ku manda.

6 Iye saganizirapo za njira ya moyo;

njira zake ndi zokhotakhota koma iye sadziwa izi.

7 Tsopano ana inu, mundimvere;

musawasiye mawu anga.

8 Uziyenda kutali ndi mkazi wotereyo,

usayandikire khomo la nyumba yake,

9 kuopa kuti ungadzalanditse ulemerero wako kwa anthu ena;

ndi zaka zako kwa anthu ankhanza,

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também