Pular para o conteúdo
Publicidade

MIYAMBO 6

6 Pita kwa nyerere, mlesi iwe;

kaonetsetse njira zake kuti uphunzirepo kanthu!

7 Zilibe mfumu,

zilibe woyangʼanira kapena wolamulira,

8 komabe zimasungiratu chakudya chake nthawi ya chilimwe

ndipo zimatuta chakudyacho nthawi yokolola.

Veja também