20 Koma,
"Ngati mdani wako ali ndi njala, mupatse chakudya.
Ngati ali ndi ludzu, mupatse kanthu kakumwa.
Pochita ichi, udzamuwunjikira makala amoto pamutu pake."
21 Musagonjetsedwe ndi choyipa, koma gonjetsani choyipa pochita chabwino.
20 Koma,
"Ngati mdani wako ali ndi njala, mupatse chakudya.
Ngati ali ndi ludzu, mupatse kanthu kakumwa.
Pochita ichi, udzamuwunjikira makala amoto pamutu pake."
21 Musagonjetsedwe ndi choyipa, koma gonjetsani choyipa pochita chabwino.