Pular para o conteúdo
Publicidade

10 versículos para enviar para a pessoa amada

Por Bíblia Online

Enviar versículos bíblicos para a pessoa amada é uma maneira especial de expressar amor, fé, compaixão e comprometimento. A Palavra de Deus fortalece os relacionamentos e oferece conforto e esperança em tempos de alegria e de dificuldade.

Em 1 Coríntios 13:4-7, Paulo nos ensina sobre o amor: "O amor é paciente, o amor é bondoso; não inveja, não se vangloria, não se orgulha."

A seguir, veja uma lista com 10 versículos bíblicos perfeitos para compartilhar com a pessoa amada.

Versículos

1. 1 Coríntios 13:4-7

Chikondi nʼcholeza mtima, chikondi nʼchokoma mtima, chilibe nsanje, sichidzikuza, sichidzitamandira. Chikondi chilibe mwano, sichodzikonda, sichipsa mtima msanga, sichisunga mangawa. Chikondi sichikondwera ndi zoyipa koma chimakondwera ndi choonadi. Chimatchinjiriza nthawi zonse, chimakhulupirika nthawi zonse, chimakhala ndi chiyembekezo nthawi zonse, chimapirira nthawi zonse.

##

2. Cantares de Salomão 8:6-7

Undiyike pamtima pako ngati chidindo,

ngati chidindo cha pa dzanja lako;

pakuti chikondi nʼchamphamvu ngati imfa,

nsanje ndiyaliwuma ngati manda.

Chikondi chimachita kuti lawilawi

ngati malawi a moto wamphamvu.

Madzi ochuluka sangachizimitse chikondi,

mitsinje singachikokolole chikondicho.

Ngati wina apereka chuma chonse

cha mʼnyumba mwake chifukwa cha chikondi,

adzangonyozeka nazo kotheratu.

Abwenzi

3. Efésios 5:25

Inu amuna, kondani akazi anu monga momwe Khristu anakondera mpingo nadzipereka yekha mʼmalo mwa mpingowo

4. 1 João 4:7

Mulungu ndiye Chikondi

Anzanga okondedwa, tiyeni tikondane wina ndi mnzake, pakuti chikondi chimachokera kwa Mulungu. Aliyense amene ali ndi chikondi ndi mwana wa Mulungu ndipo amadziwa Mulungu.

5. Colossenses 3:14

Ndipo kuwonjezera pa zonsezi valani chikondi, chimene chimangirira zonsezi pamodzi mu mgwirizano wangwiro.

6. Provérbios 17:17

Bwenzi lako limakukonda nthawi zonse,

ndipo mʼbale wako anabadwa kuti azikuthandiza pamavuto.

7. Romanos 12:10

Mukondane kwathunthu monga abale. Lemekezanani wina ndi mnzake kuposa inu eni.

8. 1 Pedro 4:8

Koposa zonse muzikondana wina ndi mnzake kwambiri, chifukwa chikondi chimaphimba machimo ambiri.

9. Filipenses 1:9

Ndipo pemphero langa ndi lakuti chikondi chanu chipitirire kukulirakulira pa chidziwitso ndi kuzama mʼmaganizo,

10. João 15:12

Lamulo langa ndi ili: Kondanani wina ndi mnzake monga Ine ndakonda inu.

Tenha um relacionamento em Deus!

A Palavra de Deus é um recurso precioso para expressar amor e encorajamento à pessoa amada. Compartilhe esses versículos para fortalecer o seu relacionamento e espalhar a luz de Cristo no seu caminhar junto a quem você ama.

Deus abençoe!

Seja o primeiro