Pular para o conteúdo
Publicidade

Os ensinamentos de Jesus sobre generosidade e desapego material

Por Bíblia Online  - 

Jesus nos ensinou que a verdadeira riqueza está em investir no Reino de Deus, não nos bens materiais. Obviamente, não estamos sendo literais, é claro que queremos que você tenha suas coisas e conquistas, mas saiba que isso é matéria, é mundando.

A riqueza que realmente engrandece sua alma, é àquela do Reino dos Céus, a riqueza da fé, do Amor de nosso Deus. Então tome cuidado com excessos, consumismo, materialismo… nada disso será bom para você, muito menos agradará a Deus.

Algumas sugestões de leitura sobre o assunto:

1. A parábola do rico insensato

Em Lucas 12:15-21, Jesus alerta contra a ganância, destacando que a vida não consiste na abundância de bens.

Kenaka Iye anawawuza kuti, "Chenjerani! Khalani tcheru ndi makhalidwe onse adyera; moyo wa munthu sukhala chifukwa cha kuchuluka kwa zimene ali nazo."

Ndipo Iye anawawuza fanizo ili, "Munda wa munthu wina wachuma unabereka kwambiri. Iye anaganiza kuti, Ndichite chiyani? Ndilibe malo osungiramo mbewu zanga.

"Ndipo Iye anati, ichi ndi chimene ndidzachite: Ndidzaphwasula nkhokwe zanga zonse ndi kumanga zokulirapo, ndipo ndidzasungira mʼmenemo mbewu ndi katundu. Ndipo ndidzawuza moyo wanga kuti, Uli nazo zinthu zabwino zambiri zimene zikhalepo zaka zambiri, usapupulume; idya, imwa ndi kukondwera.’ "

"Koma Mulungu anati kwa iye, Iwe wopusa! Usiku womwe uno moyo wako udzachotsedwa kwa iwe, ndipo ndi ndani amene adzatenge zimene iwe wadzikonzera?

"Umu ndi mmene zidzakhalire ndi aliyense amene amadziwunjikira chuma, koma si wachuma pamaso pa Mulungu."

2. "Mais bem-aventurado é dar que receber"

Atos 20:35 reforça que a generosidade é um ato de fé e obediência.

Pa zonse zimene ndinachita, ndinakuonetsani kuti pogwira ntchito molimbika motere tiyenera kuthandiza ofowoka, pokumbukira mawu a Ambuye Yesu akuti, Kupereka kumadalitsa kuposa kulandira.’ "

3. O jovem rico como exemplo de desapego

Marcos 10:21,22 nos ensina que seguir a Cristo exige abrir mão do apego material.

Yesu anamuyangʼana ndi kumukonda nati, "Ukusowa chinthu chimodzi. Pita, kagulitse zonse zimene uli nazo ndipo kapereke kwa osauka, ndipo udzakhala ndi chuma kumwamba. Ndipo ukabwere ndi kunditsata Ine."

Pa chifukwa ichi nkhope yake inagwa. Anachoka ali wachisoni, chifukwa anali ndi chuma chambiri.

Compartilhe este artigo e ajude a espalhar a Palavra de Deus conscientizando amigos e familiares.

Seja o primeiro