9 Usiku wina Ambuye anaonekera kwa Paulo mʼmasomphenya namuwuza kuti, "Usaope, pitiriza kuyankhula, usakhale chete. 10 Pakuti Ine ndili nawe, palibe aliyense amene adzakukhudza ndi kukuchitira choyipa, chifukwa mu mzinda muno ndili ndi anthu ambiri."
Publicidade
Publicidade