Pular para o conteúdo
Publicidade

Resultados da busca por "fé"

34 resultados encontrados

  1. 2 Timóteo 1

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 1
    Mostrando versículos 13–18 de 18

    13Zimene unamva kwa ine, uzisunge kuti zikhale chitsanzo cha chiphunzitso choona, mwa chikhulupiriro ndi chikondi mwa Khristu Yesu.

    14Samalira bwino zokoma zimene anakusungitsa. Uzisamalire mothandizidwa ndi Mzimu Woyera amene amakhala mwa ife.

    18Ambuye amulole kuti adzalandire chifundo kwa Ambuye pa tsiku lijalo! Ukudziwa bwino momwe iye anandithandizira mʼnjira zosiyanasiyana ku Efeso.

  2. Tiago 2

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 2
    Mostrando versículos 17–26 de 26

    17Chomwechonso, chikhulupiriro chokha chopanda ntchito zabwino ndi chakufa.

    20Munthu wopusa iwe, kodi ukufuna umboni woti chikhulupiriro chopanda ntchito zabwino nʼchakufa?

    26Monga thupi lopanda mzimu ndi lakufa, chomwechonso chikhulupiriro chopanda ntchito zabwino ndi chakufa.

  3. Gênesis 40

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 40
    Mostrando versículos 2–17 de 23

    2Farao anapsa mtima ndi akuluakulu awiriwa,

    12Yosefe anati kwa iye, "Tanthauzo lake ndi ili: Nthambi zitatuzo ndi masiku atatu.

    17Mu nsengwa yapamwamba munali zakudya zamitundumitundu za Farao, koma mbalame zimadya zakudyazo."

  4. Cânticos 1

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 1
    Mostrando versículos 2–13 de 17

    2Undipsompsone ndi milomo yakochifukwa chikondi chako nʼchokoma kuposa vinyo.

    9Iwe bwenzi langa,uli ngati kavalo wamkazi ku magaleta a Farao.

    13Wokondedwa wanga ali ngati kathumba ka mure kwa ine,kamene kamakhala pakati pa mawere angawa.

  5. Atos 24

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 24
    Mostrando versículos 3–24 de 27

    3Wolemekezeka Felike ife timazilandira zimenezi moyamika kwambiri ponseponse ndi mwa njira iliyonse.

    16Kotero ine ndimayesetsa kuti ndikhale ndi chikumbumtima chosanditsutsa pamaso pa Mulungu ndi anthu onse.

    24Patapita masiku angapo Felike anabwera pamodzi ndi mkazi wake Drusila, amene anali Myuda. Anayitana Paulo ndipo anamvetsera zimene amayankhula za chikhulupiriro mwa Khristu Yesu.

  6. Êxodo 25

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 25
    Mostrando versículos 4–27 de 40

    4Nsalu zobiriwira, zapepo, zofiira, nsalu zofewa, ubweya wambuzi;

    7miyala yokongola ya mtundu wa onikisi ndi ina yabwino yoyika pa efodi ndi pa chovala cha pachifuwa.

    27Mphetezo uziyike kufupi ndi feremu kuti azikolowekamo nsichi zonyamulira tebuloyo.

  7. Jó 6

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 6
    Mostrando versículos 6–29 de 30

    6Kodi chakudya chosakoma nʼkuchidya chopanda mchere,nanga choyera cha dzira chimakoma?

    11"Kodi mphamvu zanga nʼzotani kuti ndizikhalabe ndi chiyembekezo?Nanga zoyembekezera zanga nʼzotani kuti ndipirirebe?

    29Fewani mtima, musachite zosalungama;ganiziraninso popeza chilungamo changa chikanalipobe.

  8. 1 Reis 7

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 7
    Mostrando versículos 28–44 de 51

    28Maphakawo anapangidwa motere: Anali ndi matabwa a mʼmbali amene ankalowa mʼmaferemu.

    43maphaka khumi pamodzi ndi mabeseni khumi pa maphakawo;

    44mbiya pamodzi ndi ngʼombe khumi ndi ziwiri zazimuna zosanjikapo mbiyayo;

  9. Atos 25

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 25
    Mostrando versículos 1–22 de 27

    1Patapita masiku atatu Festo atafika mʼdera lake, anachoka ku Kaisareya ndi kupita ku Yerusalemu.

    22Ndipo Agripa anati kwa Festo, "Ine ndikufuna ndimumve ndekha munthu ameneyu." Iye anayankha kuti, "Mudzamumva mawa."

  10. Êxodo 37

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 37
    Mostrando versículos 14–20 de 29

    14Mphetezo anaziyika kufupi ndi feremu kuti azikolowekamo nsichi zonyamulira tebuloyo.

    18Mʼmbali mwake munali mphanda zisanu ndi imodzi, zitatu mbali iliyonse.

    20Pa choyikapo nyalecho panali zikho zinayi zokhala ngati maluwa amtowo, mphukira ndi maluwa ake.

  11. Atos 26

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 26
    Mostrando versículos 8–27 de 32

    8Nʼchifukwa chiyani ena a inu mukuganiza kuti nʼkosatheka kuti Mulungu aukitse akufa?

    22Koma Mulungu wakhala akundithandiza mpaka lero lino. Ine ndayima pano kuti ndichitire umboni kwa anthu onse otchuka ndi anthu wamba. Ine sindikunena zina zowonjezera koma zimene Aneneri ndi Mose ananena kuti zidzachitika.

    27Mfumu Agripa, kodi mumakhulupirira mawu a aneneri? Ine ndikudziwa kuti mumakhulupirira."

  12. Êxodo 26

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 26
    Mostrando versículos 15–28 de 37

    15"Upange maferemu amatabwa amtengo wa mkesha oyimikira chihemacho.

    18Upange maferemu makumi awiri a mbali yakummwera kwa chihemacho.

    28Mtanda wapakati pa maferemuwo uchokere pa maferemu a mbali ina mpaka mbali inanso.

  13. Êxodo 36

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 36
    Mostrando versículos 20–33 de 38

    20Iwo anapanga maferemu amatabwa amtengo wa mkesha oyimikira chihemacho.

    28ndiponso maferemu awiri a pa ngodya yakumbuyo kwenikweni kwa tenti.

    33Anapanga mtanda wapakati omwe umachokera pa maferemu a mbali ina mpaka mbali inanso.

  14. Atos 23

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 23
    Mostrando versículos 13–26 de 35

    13Anthu amene anakonza chiwembuchi analipo makumi anayi.

    25Iye analemba kalata iyi:

    26Ine Klaudiyo Lusiya,Kwa wolemekezeka, bwanamkubwa Felike:Ndikupereka moni.

Léxico (correspondência exata) Semântico (correspondência relacionada) Versículos omitidos Contexto do capítulo