1Ine ndikupereka kwa inu mlongo wathu Febe, mtumiki wa mpingo wa ku Kenkreya.
16Mupatsane moni wina ndi mnzake mwachikondi choona.Mipingo yonse ya Khristu ikupereka moni.
27kwa Mulungu yekhayo wanzeru kukhale ulemerero kwamuyaya kudzera mwa Yesu Khristu! Ameni.