Pular para o conteúdo
Publicidade

Resultados da busca por "fé"

34 resultados encontrados

  1. Romanos 16

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 16
    Mostrando versículos 1–27 de 27

    1Ine ndikupereka kwa inu mlongo wathu Febe, mtumiki wa mpingo wa ku Kenkreya.

    16Mupatsane moni wina ndi mnzake mwachikondi choona.Mipingo yonse ya Khristu ikupereka moni.

    27kwa Mulungu yekhayo wanzeru kukhale ulemerero kwamuyaya kudzera mwa Yesu Khristu! Ameni.

  2. Efésios 1

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 1
    Mostrando versículos 1–23 de 23

    1Paulo, mtumwi wa Khristu Yesu mwachifuniro cha Mulungu.Kulembera oyera mtima a ku Efeso, okhulupirika mwa Khristu Yesu:

    15Choncho, kuyambira pamene ndinamva za chikhulupiriro chanu mwa Ambuye Yesu ndi za chikondi chanu pa oyera mtima onse,

    23umene ndi thupi lake, chidzalo cha Iye amene adzaza chilichonse mu njira iliyonse.

  3. 2 Timóteo 4

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 4
    Mostrando versículos 9–22 de 22

    9Uyesetse kubwera kuno msanga.

    12Ndatumiza Tukiko ku Efeso.

    22Ambuye akhale ndi mzimu wako. Chisomo chikhale ndi inu nonse.

  4. Oséias 4

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 4
    Mostrando versículos 2–17 de 19

    2Muli kutemberera kokha, kunama ndi kupha.Kuba ndi kuchita chigololo;machimo achita kunyanyandipo akungokhalira kuphana.

    12za anthu anga.Anthu anga amapempha nzeru ku fano lamtengondipo ndodo yawo yamtengo imawayankha.Mzimu wachiwerewere umawasocheretsa;iwo sakukhulupirika kwa Mulungu wawo.

    17Efereimu waphathana ndi mafano;mulekeni!

  5. Josué 12

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 12
    Mostrando versículos 9–17 de 24

    9mfumu ya Yeriko imodzimfumu ya Ai (kufupi ndi Beteli imodzi

    16mfumu ya Makeda imodzimfumu ya Beteli imodzi

    17mfumu ya Tapuwa imodzimfumu ya Heferi imodzi

  6. Êxodo 16

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 16
    Mostrando versículos 2–36 de 36

    2Mʼchipululumo gulu lonse linadandaulira Mose ndi Aaroni

    14Mamewo atachoka, pa nthaka mʼchipululumo panaoneka tinthu tina topyapyala komanso totuwa ngati chipale.

    36(Malita awiri amafanana ndi gawo lakhumi la efa).

  7. Hebreus 11

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 11
    Mostrando versículos 4–27 de 40

    4Ndi chikhulupiriro Abele anapereka kwa Mulungu nsembe yoposa imene Kaini anapereka. Ndi chikhulupiriro anatchedwa munthu wolungama Mulungu atayamikira zopereka zake. Ngakhale iye anafa, akuyankhulabe chifukwa cha chikhulupiriro chakecho.

    24Ndi chikhulupiriro Mose atakula, anakana kutchedwa mwana wa mwana wamkazi wa Farao.

    27Ndi chikhulupiriro anachoka ku Igupto wosaopa ukali wa mfumu. Iye anapirira chifukwa anamuona Mulungu amene ndi wosaonekayo.

  8. Salmos 89

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 89
    Mostrando versículos 37–49 de 52

    37udzakhazikika kwamuyaya monga mwezi,mboni yokhulupirika mʼmitambo.Sela

    45Mwachepetsa masiku a unyamata wake;mwamuphimba ndi chofunda chochititsa manyazi.Sela

    49Inu Ambuye kodi chili kuti chikondi chanu chachikulu choyamba chija,chimene mwa kukhulupirika kwanu munalumbira kwa Davide?

  9. Efésios 3

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 3
    Mostrando versículos 12–21 de 21

    12Mwa Khristu ndi mwa chikhulupiriro chathu mwa Iye, timayandikira kwa Mulungu momasuka ndi molimbika mtima.

    17kuti Khristu akhazikike mʼmitima mwanu mwachikhulupiriro. Ndipo ndikukupemphererani kuti muzikike ndi kukhazikika mʼchikondi

    21Iyeyo akhale ndi ulemu mu mpingo ndi mwa Khristu Yesu pa mibado yonse mpaka muyaya. Ameni.

  10. Isaías 28

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 28
    Mostrando versículos 3–26 de 29

    3Ulamuliro wa atsogoleri oledzeraa ku Efereimu adzawuthetsa.

    5Tsiku limenelo Yehova Wamphamvuzonseadzakhala ngati nkhata yaufumu,chipewa chokongolakwa anthu ake otsala.

    26Mulungu wake amamulangizandi kumuphunzitsa njira yabwino.

  11. Marcos 4

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 4
    Mostrando versículos 3–18 de 41

    3"Tamverani! Mlimi anapita kukafesa mbewu zake.

    14Wofesa amafesa mawu.

    18Komabe ena, monga mbewu zofesedwa pakati pa minga, amamva mawu;

  12. Isaías 43

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 43
    Mostrando versículos 13–27 de 28

    13"Ine ndine Mulungu kuyambira nthawi yamakedzana, ndipo ndidzakhalabe Mulungu ku nthawi zonse.Palibe amene angathe kuthawa mʼmanja mwanga,ndipo chimene ndachita palibe angathe kuchisintha."

    21Anthu amene ndinadziwumbira ndekhakuti aziyimba nyimbo yotamanda Ine.

    27Kholo lanu loyamba linachimwa;ndipo Atsogoleri anu achipembedzo anandiwukira.

  13. 1 Coríntios 16

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 16
    Mostrando versículos 8–24 de 24

    8Koma ndikhala ndili ku Efeso mpaka nthawi ya Pentekosite,

    20Abale onse kuno akupereka moni wawo. Patsanani moni wachikondi chenicheni.

    24Chikondi changa chikhale ndi nonsenu mwa Khristu Yesu.

  14. Salmos 119

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 119
    Mostrando versículos 140–158 de 176

    140Mawu anu ndi woyera kwambirinʼchifukwa chake mtumiki wanune ndimawakonda.

    144Umboni wanu ndi wabwino nthawi zonse;patseni nzeru zomvetsa zinthu kuti ine ndikhale ndi moyo.Kofu

    158Ndimawayangʼana monyansidwa anthu opanda chikhulupiriro,popeza samvera mawu anu.

  15. Atos 8

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 8
    Mostrando versículos 4–35 de 40

    4Okhulupirira amene anabalalika amalalikira konse kumene amapita.

    15Atafika anawapempherera kuti alandire Mzimu Woyera,

    35Pamenepo Filipo anayambira pa malemba omwewo kumuwuza za Uthenga Wabwino wa Yesu.

  16. Colossenses 1

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 1
    Mostrando versículos 2–5 de 29

    2Kulembera abale oyera mtima ndi okhulupirira a ku Kolose mwa Khristu.Chisomo ndi mtendere kwa inu zochokera kwa Mulungu Atate athu.

    4Timayamika chifukwa tinamva za chikhulupiriro chanu mwa Khristu Yesu ndi za chikondi chanu pa oyera mtima onse.

    5Chikhulupiriro ndi chikondi, gwero lake ndi chiyembekezo chomwe muli nacho chodzalandira zimene anakusungirani kumwamba. Munamva kale za zimenezi kudzera mʼmawu a choonadi, Uthenga Wabwino

  17. Gênesis 50

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 50
    Mostrando versículos 19–23 de 26

    19Koma Yosefe anawawuza kuti, "Musachite mantha. Kodi ine ndalowa mʼmalo mwa Mulungu?

    22Yosefe anakhala mu Igupto pamodzi ndi banja lonse la abambo ake. Anakhala ndi moyo zaka 110

    23ndipo anaona mʼbado wachitatu wa ana a Efereimu. Yosefe anatenganso ana a Makiri, mwana wa Manase kukhala ngati ana a mʼbanja lake.

  18. João 1

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 1
    Mostrando versículos 2–24 de 51

    2Mawuwa anali ndi Mulungu pachiyambi.

    9Kuwunika koona kumene kuwunikira munthu aliyense kunabwera ku dziko lapansi.

    24Tsopano Afarisi ena amene anatumidwa

  19. Filipenses 4

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 4
    Mostrando versículos 20–23 de 23

    20Kwa Mulungu ndi Atate athu, kukhale ulemerero mpaka muyaya. Ameni.

    21Perekani moni kwa oyera mtima onse mwa Khristu Yesu. Abale amene ali ndi ine akupereka moni wawo.

    23Chisomo cha Ambuye Yesu Khristu chikhale ndi mzimu wanu. Ameni.

  20. Ezequiel 45

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 45
    Mostrando versículos 10–21 de 25

    10Miyeso yanu yoyezera zinthu monga efa ndi bati zizikhala zokhulupirika.

    11Efa ndi bati ikhale miyeso yolingana kukula kwake. Muyeso wa homeri ukhale wokwanira mabati khumi, ukhalenso wokwanira maefa khumi. Ndiye kuti kukula kwa miyeso iwiriyo kuzidzatsata kukula kwa homeriyo.

    21" ‘Pa tsiku la 14 la mwezi woyamba muzichita chikondwerero cha Paska, chikondwerero chake cha masiku asanu ndi awiri. Pa masiku amenewo muzidzadya buledi wopanda yisiti.

Léxico (correspondência exata) Semântico (correspondência relacionada) Versículos omitidos Contexto do capítulo