Pular para o conteúdo
Publicidade

Resultados da busca por "salvação"

75 resultados encontrados

  1. Habacuque 3

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 3
    Mostrando versículos 8–18 de 19

    8Inu Yehova, kodi munakwiyira mitsinje?Kodi munakalipira timitsinje?Kodi munapsera mtima nyanjapamene munakwera pa akavalo anundiponso magaleta anu achipulumutso?

    13Munapita kukalanditsa anthu anu,kukapulumutsa wodzozedwa wanu.Munakantha mtsogoleri wa dziko la anthu oyipa,munawononga anthu ake onse.Sela

    18komabe ine ndidzakondwera mwa Yehova,ndidzasangalala mwa Mulungu Mpulumutsi wanga.

  2. 1 Crônicas 6

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 6
    Mostrando versículos 24–51 de 81

    24Tahati, Urieli,Uziya ndi Sauli.

    30Simea, Hagiyandi Asaya.

    51Buki,Uzi, Zerahiya,

  3. Isaías 36

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 36
    Mostrando versículos 14–19 de 22

    14Zimene mfumu ikunena ndi izi: Musalole kuti Hezekiya akunamizeni. Iye sangakupulumutseni!

    18"Inu musalole kuti Hezekiya akusocheretseni pamene iye akuti, ‘Yehova adzatipulumutsa.’ Kodi alipo mulungu wa anthu a mtundu wina amene anapulumutsa dziko lake mʼdzanja la mfumu ya ku Asiriya?

    19Kodi ili kuti milungu ya Hamati ndi Aripadi? Ili kuti milungu ya Sefaravaimu? Kodi inapulumutsa Samariya mʼdzanja langa?

  4. Jó 14

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 14
    Mostrando versículos 4–14 de 22

    4Ndani angatulutse chabwino mʼchoyipa?Palibe ndi mmodzi yemwe!

    10Koma munthu amafa nayikidwa mʼmanda,amapuma mpweya wotsiriza ndipo kutha kwake nʼkomweko.

    14Munthu akafa, kodi adzakhalanso ndi moyo?Masiku anga onse a moyo wovutikawundidzadikira mpaka itafika nthawi yomasulidwa.

  5. Gênesis 49

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 49
    Mostrando versículos 3–31 de 33

    3"Rubeni, ndiwe woyamba kubadwa;mphamvu yanga ndiponso chizindikiro choyamba cha mphamvu zanga,wopambana pa ulemerero ndi mphamvu.

    18"Ndikuyembekeza chipulumutso chanu Yehova.

    31Kumeneko kunayikidwa Abrahamu ndi mkazi wake Sara, Isake ndi mkazi wake Rebeka ndipo ndinayikakonso Leya.

  6. Lucas 21

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 21
    Mostrando versículos 13–22 de 38

    13Umenewu udzakhala mwayi wanu ochitira umboni.

    19Mukadzalimbikira ndiye mudzapeze moyo.

    22Pakuti iyi ndi nthawi yachilango pokwaniritsa zonse zimene zinalembedwa.

  7. 2 Timóteo 2

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 2
    Mostrando versículos 3–10 de 26

    3Umve nane zowawa, monga msilikali wa Khristu Yesu.

    8Kumbukira Yesu Khristu wochokera ku mtundu wa Davide kuti anauka kwa akufa. Uwu ndiye uthenga wanga wabwino

    10Choncho ndikupirira chilichonse chifukwa cha osankhidwa, kuti nawonso apulumutsidwe ndi Khristu Yesu ndi kulandira ulemerero wosatha.

  8. Números 33

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 33
    Mostrando versículos 15–22 de 56

    15Atachoka ku Refidimu anakamanga ku chipululu cha Sinai

    21Atachoka ku Libina anakamanga ku Risa.

    22Atachoka ku Risa anakamanga ku Kehelata.

  9. Provérbios 14

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 14
    Mostrando versículos 12–27 de 35

    12Pali njira ina yooneka ngati yabwino kwa munthu,koma kumatsiriziro kwake ndi ku imfa.

    25Mboni yokhulupirika imapulumutsa miyoyo,koma mboni yabodza imaphetsa.

    27Kuopa Yehova ndiye kasupe wamoyo,kumathandiza munthu kuti apewe msampha wa imfa.

  10. 2 Tessalonicenses 1

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 1
    Mostrando versículos 1–7 de 12

    1Paulo, Silivano ndi Timoteyo.Kulembera mpingo wa ku Tesalonika, umene uli mwa Mulungu Atate athu ndi Ambuye Yesu Khristu.

    6Mulungu ndi wolungama ndipo adzalanga amene amakusautsaniwo

    7ndikukupatsani mpumulo amene mukusautsidwa, pamodzi ndi ifenso. Izi zidzachitika Ambuye Yesu akadzaoneka mʼmalawi amoto kuchokera kumwamba pamodzi ndi angelo ake amphamvu.

  11. 1 Coríntios 15

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 15
    Mostrando versículos 26–53 de 58

    26Mdani wotsiriza kuwonongedwa ndi imfa.

    36Wopusa iwe! Chimene mudzala sichikhala ndi moyo pokhapokha chitayamba chafa.

    53Pakuti chovunda chiyenera kuvala chosavunda, ndi thupi ili lakufa liyenera kuvala losafa.

  12. Ezequiel 7

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 7
    Mostrando versículos 6–25 de 27

    6Chimaliziro chafika!Chimaliziro chafika!Chiwonongeko chakugwera.Taona chafika!

    11Chiwawa chasanduka ndodoyowakwapulira chifukwa cha kuyipa kwawo.Palibe mwa anthu amenewo amene adzatsale.Palibe ndi mmodzi yemwe mwa unyinji wawo.Palibiretu ndipo sipadzapezekamunthu wowalira maliro.

    25Nkhawa ikadzawafikiraadzafunafuna mtendere koma osawupeza.

  13. Esdras 10

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 10
    Mostrando versículos 32–42 de 44

    32Benjamini, Maluki ndi Semariya.

    37Mataniya, Matenayi ndi Yasu.

    42Salumu, Amariya ndi Yosefe.

  14. Josué 15

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 15
    Mostrando versículos 26–40 de 63

    26Amamu, Sema, Molada

    31Zikilagi, Madimena, Sanisana,

    40Kaboni, Lahimasi, Kitilisi,

  15. Deuteronômio 23

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 23
    Mostrando versículos 1–12 de 25

    1Mwamuna aliyense wofulidwa kapena woduka chiwalo chachimuna asalowe nawo mu msonkhano wa Yehova.

    11Koma dzuwa likapendeka ayenera kusamba ndipo polowa dzuwa akhoza kubwerera ku msasa.

    12Mukonze malo kunja kwa msasa kumene mukhoza kukadzithandizirako.

  16. 2 Samuel 22

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 22
    Mostrando versículos 2–47 de 51

    2Iye anati,"Yehova ndiye thanthwe langa, chitetezo changa ndi mpulumutsi wanga.

    3Mulungu wanga ndiye thanthwe langa, mʼmene ndimathawiramo,chishango changa ndi ndodo yachipulumutso changa.Iye ndi linga langa, pothawirapo panga ndi mpulumutsi wanga.Munandipulumutsa mʼmanja mwa anthu ankhanza.

    47"Yehova ndi wamoyo! Litamandidwe Thanthwe langa.Akuzike Mulungu, Thanthwe, Mpulumutsi wanga!

  17. Romanos 6

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 6
    Mostrando versículos 1–7 de 23

    1Nanga tinene chiyani? Kodi tipitirire kuchimwa kuti chisomo chichulukebe?

    3Kodi simukudziwa kuti tonse amene tinabatizidwa mwa Khristu Yesu tinabatizidwa mu imfa yake?

    7chifukwa aliyense amene anafa anamasuka ku tchimo.

  18. Hebreus 2

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 2
    Mostrando versículos 3–18 de 18

    3Nanga ife tidzapulumuka bwanji tikapanda kusamala chipulumutso chachikulu chotere? Ambuye ndiye anayamba kuyankhula za chipulumutsochi, kenaka amenenso anamvawo anatitsimikizira.

    10Mulungu amene analenga zinthu zonse ndipo zinthu zonse zilipo chifukwa cha Iye ndi mwa Iye, anachiona choyenera kubweretsa ana ake ambiri mu ulemerero. Kunali koyenera kudzera mʼnjira ya zowawa, kumusandutsa Yesu mtsogoleri wangwiro, woyenera kubweretsa chipulumutso chawo.

    18Popeza Iye mwini anamva zowawa pamene anayesedwa, Iyeyo angathe kuthandiza amene akuyesedwanso.

  19. Efésios 4

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 4
    Mostrando versículos 3–26 de 32

    3Muyesetse kusunga umodzi wa Mzimu; umodzi umene umatimangirira pamodzi mu mtendere.

    5Pali Ambuye mmodzi, chikhulupiriro chimodzi, ubatizo umodzi;

    26Kwiyani koma musachimwe. Dzuwa lisalowe mukanali chikwiyire.

  20. João 10

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 10
    Mostrando versículos 2–39 de 42

    2Munthu amene amalowera pa khomo ndi mʼbusa wankhosazo.

    19Pa mawu awa Ayuda anagawikananso.

    39Iwo anafuna kumugwiranso koma anawapulumuka mʼmanja mwawo.

Léxico (correspondência exata) Semântico (correspondência relacionada) Versículos omitidos Contexto do capítulo