8Inu Yehova, kodi munakwiyira mitsinje?Kodi munakalipira timitsinje?Kodi munapsera mtima nyanjapamene munakwera pa akavalo anundiponso magaleta anu achipulumutso?
13Munapita kukalanditsa anthu anu,kukapulumutsa wodzozedwa wanu.Munakantha mtsogoleri wa dziko la anthu oyipa,munawononga anthu ake onse.Sela
18komabe ine ndidzakondwera mwa Yehova,ndidzasangalala mwa Mulungu Mpulumutsi wanga.