Pular para o conteúdo
Publicidade

Resultados da busca por "salvação"

78 resultados encontrados

  1. Salmos 3

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 3
    Mostrando versículos 2–8 de 8

    2Ambiri akunena za ine kuti,"Mulungu sadzamupulumutsa."Sela

    7Dzukani, Inu Yehova!Pulumutseni, Inu Mulungu wanga.Akantheni adani anga onse pa msagwada;gululani mano a anthu oyipa.

    8Chipulumutso chimachokera kwa Yehova.Madalitso akhale pa anthu anu.Sela

  2. Jó 33

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 33
    Mostrando versículos 18–30 de 33

    18kumulanditsa munthu ku manda,kuti moyo wake usawonongeke ndi lupanga.

    28Iye anapulumutsa moyo wanga kuti usapite ku manda,ndipo ndidzakhala ndi moyo ndi kuonanso kuwala kwa dzuwa.’

    30kupulumutsa moyo wa munthuyo ku manda,kuti athe kuonanso kuwala kwa moyo.

  3. Romanos 7

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 7
    Mostrando versículos 9–24 de 25

    9Nthawi ina ndinali ndi moyo popanda Malamulo. Koma nditayamba kudziwa Malamulo, pomwepo uchimo unayamba kuphuka,

    12Choncho lamulo ndi loyera, lolungama ndi labwino.

    24Kalanga ine! Adzandipulumutsa ndani ku thupi la imfali?

  4. Provérbios 23

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 23
    Mostrando versículos 11–14 de 35

    11paja Mpulumutsi wawo ndi wamphamvu;iye adzawateteza pa milandu yawo kutsutsana nawe.

    13Usaleke kumulangiza mwana;ngati umulanga ndi chikwapu sadzafa.

    14Ukamukwapula ndi tsatsaudzapulumutsa moyo wake.

  5. Mateus 18

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 18
    Mostrando versículos 4–11 de 35

    4Chifukwa chake, aliyense amene adzichepetsa yekha ngati kamwana aka, ameneyo ndiye wamkulu koposa onse mu ufumu wakumwamba.

    8Ngati dzanja lako kapena phazi lako likuchimwitsa, lidule ndi kulitaya. Ndi bwino kwa iwe kulowa mʼmoyo wosatha wolumala kusiyana ndi kukhala ndi manja awiri kapena mapazi awiri ndi kukaponyedwa ku moto wosatha.

    11(Mwana wa Munthu anabwera kudzapulumutsa chimene chinatayika).

  6. Salmos 18

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 18
    Mostrando versículos 2–46 de 50

    2Yehova ndiye thanthwe langa, chitetezo changa ndi mpulumutsi wanga;Mulungu wanga ndi thanthwe langa mʼmene ndimathawiramo.Chishango changa ndi ndodo yachipulumutso changa, ndi linga langa.

    19Iye anandipititsa kumalo otakasuka;anandipulumutsa chifukwa amakondwera nane.

    46Yehova ndi wamoyo! Litamandidwe Thanthwe langa!Akuzike Mulungu Mpulumutsi wanga!

  7. Lamentações 3

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 3
    Mostrando versículos 26–35 de 66

    26nʼkwabwino kudikira chipulumutso chaYehova modekha.

    27Nʼkwabwino kuti munthu asenze golipamene ali wamngʼono.

    35kukaniza munthu ufulu wakepamaso pa Wammwambamwamba,

  8. Mateus 24

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 24
    Mostrando versículos 8–20 de 51

    8Zonsezi ndi chiyambi chabe cha zowawa.

    13koma wopirira kufikira chimaliziro adzapulumuka.

    20Pempherani kuti kuthawa kwanu kusadzachitike nthawi yozizira kapena pa Sabata.

  9. 1 Pedro 1

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 1
    Mostrando versículos 4–9 de 25

    4kuti tidzalandire chuma chomwe sichingawonongeke, kuyipitsidwa kapena kufota. Chuma chimenechi akukusungirani kumwamba.

    5Mwachikhulupiriro, mukusungidwa ndi mphamvu ya Mulungu mpaka chipulumutso chitafika chimene chinakonzedwa kuti adzachionetse nthawi yotsiriza.

    9Motero mukulandira mphotho ya chikhulupiriro chanu, ndiyo chipulumutso cha moyo wanu.

  10. Deuteronômio 5

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 5
    Mostrando versículos 17–26 de 33

    17"Usaphe.

    19"Usabe.

    26Pakuti ndi munthu uti wolengedwa amene anamvapo mawu a Mulungu wamoyo akuyankhula kuchokera mʼmoto, monga tachitiramu, nakhala ndi moyo?

  11. Lucas 20

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 20
    Mostrando versículos 30–35 de 47

    30Wachiwiri

    32Pa mapeto pake mkaziyo anafanso.

    35Koma mʼmoyo umene ukubwerawo, anthu amene adzaukitsidwe kwa akufa sadzakwatira kapena kukwatiwa.

  12. Levítico 1

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 1
    Mostrando versículos 4–13 de 17

    4Munthuyo asanjike dzanja lake pa mutu pa nsembe yopserezayo, ndipo idzalandiridwa kuti ikhale yopepesera machimo ake.

    6Munthuyo asende nsembe yopserezayo ndi kuyidula nthulinthuli.

    13Munthuyo atsuke zamʼkati mwa nyamayo pamodzi ndi miyendo yake yomwe, ndipo wansembe abwere nazo zonse ndi kuzitentha pa guwa. Iyi ndi nsembe yopsereza, chopereka chotentha pa moto, fungo lokomera Yehova.

  13. Cânticos 2

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 2
    Mostrando versículos 1–15 de 17

    1Ine ndine duwa la ku Saroni,duwa lokongola la ku zigwa.Mwamuna

    2Monga duwa lokongola pakati pa mingandi momwe alili wokondedwa wanga pakati pa atsikana.Mkazi

    15Mutigwirire nkhandwe,nkhandwe zingʼonozingʼonozimene zikuwononga minda ya mpesa,minda yathu ya mpesa imene yayamba maluwa.Mkazi

  14. Números 6

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 6
    Mostrando versículos 8–25 de 27

    8Munthuyo ndi wopatulika masiku onse odzipereka kwake kwa Yehova.

    24" ‘Yehova akudalitsendi kukusunga;

    25Yehova awalitse nkhope yake pa iwe,nakuchitira chisomo;

  15. Efésios 6

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 6
    Mostrando versículos 11–17 de 24

    11Valani zida zonse za Mulungu kuti muthe kuyima ndi kukana machenjerero a Satana.

    15Valani Uthenga Wabwino wamtendere ku mapazi anu ngati nsapato.

    17Valani chipewa cha chipulumutso ndi kutenga lupanga la mzimu, limene ndi Mawu a Mulungu.

  16. Êxodo 20

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 20
    Mostrando versículos 8–15 de 26

    8"Uzisunga tsiku la Sabata kuti likhale lopatulika.

    13"Usaphe.

    15"Usabe.

  17. Jeremias 20

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 20
    Mostrando versículos 4–14 de 18

    4Pakuti Yehova akuti, ‘Ndidzakusandutsa choopsa kwa mwiniwakewe ndi kwa abwenzi ako onse; iweyo ukuona. Anthu a ku Yuda ndidzawapereka onse mʼmanja mwa mfumu ya ku Babuloni. Ena adzatengedwa ukapolo ku Babuloni ndipo ena adzaphedwa pa nkhondo.

    13Imbirani Yehova!Mutamandeni Yehova!Iye amapulumutsa wosaukamʼmanja mwa anthu oyipa.

    14Litembereredwe tsiku limene ndinabadwa!Tsiku limene amayi anga anandibereka lisatamandidwe!

  18. Jeremias 48

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 48
    Mostrando versículos 6–22 de 47

    6Thawani! Dzipulumutseni;khalani ngati mbidzi ya mʼchipululu.

    10"Wotembereredwa munthu amene amagwira ntchito ya Yehova monyinyirika!Wotembereredwa munthu amene amaletsa lupanga lake kupha anthu!

    22Diboni, Nebo, Beti-Dibilataimu,

  19. Neemias 10

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 10
    Mostrando versículos 12–25 de 39

    12Zakuri, Serebiya, Sebaniya,

    20Magipiyasi, Mesulamu, Heziri

    25Rehumu, Hasabiya, Maaseya,

  20. Gênesis 49

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 49
    Mostrando versículos 3–31 de 33

    3"Rubeni, ndiwe woyamba kubadwa;mphamvu yanga ndiponso chizindikiro choyamba cha mphamvu zanga,wopambana pa ulemerero ndi mphamvu.

    18"Ndikuyembekeza chipulumutso chanu Yehova.

    31Kumeneko kunayikidwa Abrahamu ndi mkazi wake Sara, Isake ndi mkazi wake Rebeka ndipo ndinayikakonso Leya.

Léxico (correspondência exata) Semântico (correspondência relacionada) Versículos omitidos Contexto do capítulo