19 Muziyankhulana wina ndi mnzake mawu a Masalimo, nyimbo za Mulungu ndi nyimbo za uzimu. Muziyimbira Ambuye movomerezana ndi mitima yanu. 20 Muziyamika Mulungu Atate nthawi zonse chifukwa cha zonse, mʼdzina la Ambuye athu Yesu Khristu.
Malangizo kwa Akazi ndi Amuna Mʼbanja
21 Gonjeranani wina ndi mnzake, kuonetsa kuopa Khristu.