Kukhazikitsidwa kwa Paska
1 Yehova anayankhula kwa Mose ndi Aaroni mʼdziko la Igupto kuti,
30 Farao ndi nduna zake zonse ndiponso Aigupto onse anadzuka pakati pa usiku, ndipo kunali kulira kwakukulu mʼdziko lonse la Igupto, pakuti panalibe nyumba imene munalibe munthu wakufa.