4 Pamenepo anandiwuza kuti, "Lengeza kwa mafupa amenewa ndi kuwawuza kuti amve mawu a Ine Yehova! 5 Uwawuze kuti zimene Ine Ambuye Yehova ndikunena kwa mafupa ndi izi: Ndidzawuzira mpweya mwa inu, ndipo mudzakhalanso ndi moyo.
Publicidade
4 Pamenepo anandiwuza kuti, "Lengeza kwa mafupa amenewa ndi kuwawuza kuti amve mawu a Ine Yehova! 5 Uwawuze kuti zimene Ine Ambuye Yehova ndikunena kwa mafupa ndi izi: Ndidzawuzira mpweya mwa inu, ndipo mudzakhalanso ndi moyo.