Pular para o conteúdo
Publicidade

GENESIS 41

38 Choncho Farao anafunsa nduna zake nati, "Kodi tingathe kumupeza munthu wina ngati uyu, amene ali ndi mzimu wa Mulungu?"

39 Farao anati kwa Yosefe, "Pakuti Mulungu wakudziwitsa iwe zonsezi, palibe wina wodziwa zinthu ndi wanzeru ngati iwe.

Veja também