Publicidade

Hebreus 12

Mulungu Amalanga Ana ake

5 Kodi mwayiwala mawu olimbitsa mtima aja, amene Mulungu anayankhula kwa inu ngati ana ake? Mawuwo ndi awa:

"Mwana wanga, usapeputse kulanga kwa Ambuye

ndipo usataye mtima pamene akukudzudzula.

6 Chifukwa Ambuye amadzudzula amene amawakonda

ndipo amalanga aliyense amene amamulandira."

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-29_22-07-56-