Mulungu Amalanga Ana ake
5 Kodi mwayiwala mawu olimbitsa mtima aja, amene Mulungu anayankhula kwa inu ngati ana ake? Mawuwo ndi awa:
"Mwana wanga, usapeputse kulanga kwa Ambuye
ndipo usataye mtima pamene akukudzudzula.
6 Chifukwa Ambuye amadzudzula amene amawakonda
ndipo amalanga aliyense amene amamulandira."