Pular para o conteúdo
Publicidade

AHEBRI 12

Mulungu Amalanga Ana ake

5 Kodi mwayiwala mawu olimbitsa mtima aja, amene Mulungu anayankhula kwa inu ngati ana ake? Mawuwo ndi awa:

"Mwana wanga, usapeputse kulanga kwa Ambuye

ndipo usataye mtima pamene akukudzudzula.

6 Chifukwa Ambuye amadzudzula amene amawakonda

ndipo amalanga aliyense amene amamulandira."

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também