5 Mtima wanu usakonde ndalama koma mukhutitsidwe ndi zimene muli nazo, chifukwa Mulungu anati,
"Sadzakusiyani,
kapena kukutayani konse."
6 Kotero ife tikunena molimba mtima kuti,
"Ambuye ndiye mthandizi wanga;
sindidzachita mantha. Munthu angandichitenji ine?"