Pular para o conteúdo
Publicidade

Jó 29

12 chifukwa ndinkapulumutsa mʼmphawi wofuna chithandizo,

ndiponso mwana wamasiye amene analibe aliyense womuthandiza.

13 Munthu amene anali pafupi kufa ankandidalitsa;

ndinkasangalatsanso mkazi wamasiye.

Veja também