12 chifukwa ndinkapulumutsa mʼmphawi wofuna chithandizo,
ndiponso mwana wamasiye amene analibe aliyense womuthandiza.
13 Munthu amene anali pafupi kufa ankandidalitsa;
ndinkasangalatsanso mkazi wamasiye.
12 chifukwa ndinkapulumutsa mʼmphawi wofuna chithandizo,
ndiponso mwana wamasiye amene analibe aliyense womuthandiza.
13 Munthu amene anali pafupi kufa ankandidalitsa;
ndinkasangalatsanso mkazi wamasiye.