Publicidade

João 19

4 Pilato anatulukanso ndipo anati kwa Ayuda, "Taonani, ine ndikumubweretsa kuti inu mudziwe kuti ine sindikupeza chifukwa chomuyimbira mlandu." 5 Pamenepo Yesu anatuluka atavala nkhata yaminga ndi mkanjo wapepo ndipo Pilato anawawuza kuti, "Nayu munthu uja!"

6 Atangomuona Iye akulu a ansembe ndi akuluakulu ena anafuwula kuti, "Mpachikeni! Mpachikeni!"

Koma Pilato anayankha kuti, "Inu mutengeni ndi kumupachika. Koma ine sindikupeza chifukwa chomuyimbira mlandu."

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-29_22-07-56-