16 Ndipo anthu anayankha, "Sizingatheke kuti timusiye Yehova ndi kutumikira milungu ina! 17 Yehova Mulungu wathu ndiye amene anatitulutsa ife ndi makolo athu mu ukapolo, mʼdziko la Igupto. Tinaona ndi maso athu zizindikiro zozizwitsa zimene anachita. Iye anatiteteza pa ulendo wathu wonse ndi pakati pa mitundu yonse imene tinkakumana nayo.
Publicidade
Publicidade