Pular para o conteúdo
Publicidade

Jó 1

21 nati,

"Ndinatuluka maliseche mʼmimba mwa amayi anga,

namonso mʼmanda ndidzalowa wamaliseche.

Yehova ndiye anapereka ndipo Yehova watenga;

litamandike dzina la Yehova."

22 Mu zonsezi, Yobu sanachimwe kapena kunena kuti, "Mulungu walakwa."

Veja também