10 Koma Iye amadziwa mmene ndimayendera;
Iyeyo akandiyesa adzandipeza kuti ndili ngati golide.
11 Mapazi anga akhala akuponda mʼmapazi ake;
ndasunga njira yake ndipo sindinayitaye.
10 Koma Iye amadziwa mmene ndimayendera;
Iyeyo akandiyesa adzandipeza kuti ndili ngati golide.
11 Mapazi anga akhala akuponda mʼmapazi ake;
ndasunga njira yake ndipo sindinayitaye.