14 Zimenezi ndi pangʼono chabe mwa ntchito yake;
tingomva pangʼono za Iye ngati kunongʼona!
Kodi ndani angathe kudziwa kukula kwa mphamvu zake?"
14 Zimenezi ndi pangʼono chabe mwa ntchito yake;
tingomva pangʼono za Iye ngati kunongʼona!
Kodi ndani angathe kudziwa kukula kwa mphamvu zake?"