Pular para o conteúdo
Publicidade

Mateus 10

35 Pakuti Ine ndabwera kudzalekanitsa

" Munthu ndi abambo ake,

mwana wamkazi ndi amayi ake,

mtengwa kulekanitsidwa ndi apongozi ake,

36 adani a munthu adzakhala a mʼbanja mwake momwe.

Veja também