Pular para o conteúdo
Publicidade

Mateus 18

Za Mʼbale Amene Akuchimwirani

15 "Ngati mʼbale wako akuchimwira, pita kamuwuze cholakwa chake pa awiri. Ngati akumvera, wamubweza mʼbale wakoyo. 16 Koma ngati sakumvera, katenge wina mmodzi kapena ena awiri, kuti nkhani itsimikizike ndi umboni wa anthu awiri kapena atatu.

Veja também