26 Pamene ankadya, Yesu anatenga buledi, nayamika ndipo anamunyema nagawira ophunzira ake nanena kuti, "Tengani, idyani; ili ndi thupi langa."
27 Kenaka anatenga chikho, nayamika nachipereka kwa iwo nati, "Imwani nonsenu. 28 Awa ndi magazi anga a pangano amene akhetsedwa chifukwa cha ambiri kuti akhululukidwe machimo.