Pular para o conteúdo
Publicidade

Mateus 3

Kubatizidwa kwa Yesu

13 Pamenepo Yesu anabwera kuchokera ku Galileya kudzabatizidwa ndi Yohane mu mtsinje wa Yorodani.

17 Ndipo mawu anamveka kuchokera kumwamba kuti, "Uyu ndiye mwana wanga wokondedwa amene ndikondwera naye."

Veja também