Pular para o conteúdo
Publicidade

MATEYU 5

Zokhudza Kusudzula Mkazi

31 "Ananena kuti, Aliyense wosudzula mkazi wake ayenera amupatse kalata ya chisudzulo. 32 Koma Ine ndikukuwuzani kuti aliyense amene asudzula mkazi wake pa chifukwa china chilichonse osati chifukwa cha chiwerewere, akumuchititsa mkaziyo chigololo ndipo aliyense wokwatira mkaziyo, akuchitanso chigololo.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também