Pular para o conteúdo
Publicidade

NEHEMIYA 2

17 Ndinawawuza kuti, "Inu mukuona mavuto amene tili nawo. Mukuona kuti mzinda wa Yerusalemu wasanduka bwinja ndipo zipata zake zatenthedwa ndi moto. Tsono tiyeni timangenso makoma a Yerusalemu ndipo sitidzachitanso manyazi." 18 Ndinawawuza za mmene Yehova Mulungu wanga anandichitira zabwino ndiponso mawu amene mfumu inandiwuza.

Tsono anati, "Tiyeni tiyambenso kumanga." Kotero analimbitsana mtima kuti ayambenso ntchito yabwinoyi.

Veja também