Pular para o conteúdo
Publicidade

MIYAMBO 1

Malangizo kuti Asunge Nzeru

Malangizo kwa Achinyamata

8 Mwana wanga, mvera malangizo a abambo ako

ndipo usakane mawu okuwongolera a amayi ako.

9 Ali ngati sangamutu yokongola ya maluwa pamutu pako

ndiponso ali ngati mkanda mʼkhosi mwako.

Estes versículos te tocaram? Ore agora!

+581 estão orando agora.

Junte-se à corrente de oração.

Veja também