13 Munthu woyipa amakodwa mu msampha wa mayankhulidwe ake oyipa;
koma munthu wolungama amatuluka mʼmavuto.
17 Woyankhula zoona amapereka umboni woona,
koma mboni yabodza imafotokoza zonama.
13 Munthu woyipa amakodwa mu msampha wa mayankhulidwe ake oyipa;
koma munthu wolungama amatuluka mʼmavuto.
17 Woyankhula zoona amapereka umboni woona,
koma mboni yabodza imafotokoza zonama.