25 Mphamvu ndi ulemu zimakhala ngati chovala chake;
ndipo amaseka osaopa zamʼtsogolo.
26 Iye amayankhula mwanzeru,
amaphunzitsa anthu mwachikondi.
25 Mphamvu ndi ulemu zimakhala ngati chovala chake;
ndipo amaseka osaopa zamʼtsogolo.
26 Iye amayankhula mwanzeru,
amaphunzitsa anthu mwachikondi.