Publicidade

Provérbios 8

32 "Ndiye tsono ana inu, ndimvereni;

odala anthu amene amasunga njira zanga.

33 Mverani malangizo anga kuti mukhale ndi nzeru;

musanyozere mawu anga.

Veja também

Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-07-04_21-26-40-