Publicidade

Romanos 9

20 Koma ndiwe yani, munthu wamba, woti nʼkutsutsana ndi Mulungu? "Kodi chimene chinawumbidwa nʼkufunsa amene anachiwumba kuti, Kodi unandiwumbiranji motere?’ " 21 Kodi wowumba alibe ufulu wowumba kuchokera ku dothi lomwelo mbiya yamtengowapatali ndi ina yamtengo wotsika?

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-28_14-13-17-