20 Koma ndiwe yani, munthu wamba, woti nʼkutsutsana ndi Mulungu? "Kodi chimene chinawumbidwa nʼkufunsa amene anachiwumba kuti, ‘Kodi unandiwumbiranji motere?’ " 21 Kodi wowumba alibe ufulu wowumba kuchokera ku dothi lomwelo mbiya yamtengowapatali ndi ina yamtengo wotsika?
Publicidade
Publicidade