O poder da oração de intercessão: orando pelos outros
A oração de intercessão é um dos atos mais poderosos que podemos fazer como cristãos. Interceder por outros é uma maneira de mostrar amor e cuidado, e também de se envolver na obra de Deus em favor dos outros.
Na Bíblia, vemos diversos exemplos de intercessão, desde os grandes profetas até Jesus Cristo, que intercedeu por nós...
O exemplo de Jesus como intercessor
Jesus Cristo é o exemplo perfeito de intercessor. Em João 17, Ele faz uma oração profunda em favor de Seus discípulos, pedindo a Deus que os guarde e os proteja do mal. Ele também intercede por aqueles que ainda creriam n'Ele, mostrando a importância de orar pelos outros, mesmo antes que eles soubessem de suas necessidades.
Jesus, em Sua vida, ensinou que a oração não é apenas para nossos próprios interesses, mas também para o bem-estar dos outros.
Yesu Adzipempherera Yekha
Yesu atatha kunena izi, anayangʼana kumwamba ndipo anapemphera:
"Atate, nthawi yafika. Lemekezani Mwana wanu, kuti Mwana wanuyo akulemekezeni Inu. Pakuti Inu munamupatsa Iye ulamuliro pa anthu onse kuti apereke moyo wosatha kwa onse amene mwamupatsa. Tsono moyo wosathawo ndi uwu: Iwo akudziweni Inu, Mulungu yekhayo woona, ndi Yesu Khristu, amene Inu mwamutuma. Ine ndabweretsa ulemerero wanu pa dziko pamene ndamaliza ntchito imene munandipatsa kuti ndi igwire. Ndipo tsopano, Atate, ndilemekezeni Ine pamaso panu ndi ulemerero uja umene ndinali nawo kwa Inu dziko lapansi lisanayambe.
Yesu Apempherera Ophunzira Ake
"Ine ndawadziwitsa za Inu anthu amene munandipatsa mʼdziko lapansi. Iwo anali anu. Inu munawapereka kwa Ine ndipo amvera mawu anu. Tsopano akudziwa kuti zonse zimene munandipatsa nʼzochokera kwa Inu. Pakuti Ine ndiwapatsa mawu amene Inu munandipatsa ndipo awalandira. Iwo akudziwa ndithu kuti Ine ndinachokera kwa Inu, ndipo akukhulupirira kuti Inu ndiye amene munandituma Ine. Ine ndikuwapempherera. Ine sindikupempherera dziko lapansi, koma anthu amene Inu mwandipatsa, pakuti ndi anu. Zonse zimene Ine ndili nazo ndi zanu, ndipo zonse zimene Inu muli nazo ndi zanga. Choncho Ine ndalemekezedwa mwa iwowo. Ine sindikukhalanso mʼdziko lapansi nthawi yayitali, koma iwo akanali mʼdziko lapansi. Ine ndikubwera kwa Inu. Atate Woyera, atetezeni ndi mphamvu za dzina lanu. Dzina limene munandipatsa Ine, kuti iwo akhale amodzi monga Ife tili amodzi. Pamene ndinali nawo, ndinawateteza ndi kuwasunga mosamala mʼdzina limene munandipatsa. Palibe ndi mmodzi yemwe amene anatayika kupatula yekhayo amene anayenera kuwonongeka kuti malemba akwaniritsidwe.
"Tsopano ndikubwera kwa Inu. Ndikunena izi ndikanali mʼdziko lapansi, kuti iwo akhale ndi muyeso wodzaza wachimwemwe changa mʼkati mwawo. Ine ndawapatsa mawu anu ndipo dziko lapansi likudana nawo, pakuti sali a dziko lapansi monga Ine sindilinso wa dziko lapansi. Sindikupempha kuti muwachotse mʼdziko lapansi koma kuti muwateteze kwa woyipayo. Iwo si a dziko lapansi, monga Ine sindilinso wa dziko lapansi. Ayeretseni ndi choonadi chanu. Mawu anu ndiye choonadi. Monga Inu munandituma Ine mʼdziko lapansi, Inenso ndikuwatuma mʼdziko lapansi. Chifukwa cha iwowa Ine ndikudziyeretsa, kuti iwo ayeretsedwenso kwenikweni.
Yesu Apempherera Okhulupirira Onse
"Ine sindikupempherera iwo okhawa, komanso amene adzandikhulupirira chifukwa cha uthenga wawo. Ndikuwapempherera kuti onsewa akhale amodzi. Monga Inu Atate muli mwa Ine ndi Ine mwa Inu, iwonso akhale mwa Ife kuti dziko lapansi likhulupirire kuti Inu munandituma Ine. Ine ndawapatsa ulemerero umene munandipatsa Ine, kuti akhale amodzi monga Ife tili amodzi. Ine ndikhale mwa iwo ndipo Inu mwa Ine kuti umodzi wawo ukhale wangwiro. Choncho dziko lapansi lidzadziwa kuti Inu munandituma Ine ndipo Inu mwawakonda iwowa monga momwe Inu munandikondera Ine.
"Atate, Ine ndikufuna kuti anthu amene mwandipatsa Ine adzakhale ndi Ine kumene kuli Ine, ndi kuona ulemerero wanga, ulemerero umene munandipatsa chifukwa Inu munandikonda dziko lapansi lisanalengedwe.
"Atate wolungama, ngakhale kuti dziko lapansi silikudziwani Inu, Ine ndimakudziwani, ndipo iwo amadziwa kuti Inu munandituma Ine. Ine ndawadziwitsa dzina lanu, ndipo ndidzapitiriza kuwadziwitsa dzina lanulo, kuti chikondi chomwe munandikonda nacho chikhale mwa iwo, ndipo Ine mwa iwo."
Intercessão no Antigo Testamento
O Antigo Testamento também traz exemplos poderosos de intercessão. Moisés intercedeu pelo povo de Israel quando eles pecaram contra Deus, e Deus ouviu sua oração e poupou a nação (Êxodo 32:11-14). Da mesma forma, Abraão intercedeu por Sodoma e Gomorra, buscando que Deus poupasse as cidades se houvesse pelo menos dez justos (Gênesis 18:23-33).
Esses exemplos nos ensinam que podemos ir diante de Deus em favor dos outros, pedindo Sua misericórdia e intervenção em suas vidas.
A importância da intercessão na vida cristã
Interceder pelos outros é um reflexo do nosso amor e preocupação com eles. A Bíblia nos ensina a orar uns pelos outros (Tiago 5:16), e a oração de intercessão é uma maneira de demonstrar esse amor. Além disso, a intercessão fortalece nossa própria fé, pois nos permite ver como Deus atua na vida das pessoas de maneiras que muitas vezes não conseguimos compreender.
Quando oramos pelos outros, também estamos colaborando com Deus em Sua obra redentora no mundo.
Versículos que incentivam a oração de intercessão:
1. 1 Timóteo 2:1: "Antes de tudo, exorto que se façam deprecações, orações, intercessões e ações de graças por todos os homens."
2. Romanos 8:34: "Quem os condenará? Foi Cristo Jesus quem morreu, e mais, quem ressuscitou, está à direita de Deus e também intercede por nós."
3. Efésios 6:18: "Com toda oração e súplica, orando em todo o tempo no Espírito, e para isso vigiando com toda a perseverança e súplica por todos os santos."
O impacto da oração de intercessão
Quando oramos pelos outros, Deus pode agir de maneiras que não conseguimos prever, trazendo cura, proteção, e direção a quem precisa. A oração de intercessão tem um grande poder, pois nos conecta diretamente com o coração de Deus para os outros, e Ele honra nossas orações.
Lembre-se, não importa se a pessoa está perto ou distante, a oração pode atravessar qualquer barreira. Se este artigo te ajudou, compartilhe e espalhe a Palavra de Deus.