Pular para o conteúdo
Publicidade

Seguir a Jesus

Por Bíblia Online

Seguir a Jesus é o convite mais transformador da Bíblia. Jesus chamou pescadores, cobradores de impostos e pessoas comuns para deixar tudo e segui-lo. Esse chamado continua vivo hoje.

O chamado de Jesus

Jesus disse: 'Segue-me'. Esse convite simples e poderoso mudou a vida de pescadores, publicanos e pessoas comuns ao longo da história.

Yesu wadaakambila, "Majhani nichateni! Nane sinikuchiteni mukhale opeleka wandhu kwa Mnungu." Pampajha adayasiya makoka yao niadamchata.

Yesu wamtana Matayo

Yesu wadachokapo pamenepo, ni yapo wamachoka wadamuona mundhu mwina wolandila malipilo uyo watanidwa Matayo, wakhala mnyumba ya malipilo. Yesu wadamtana ni kumkambila, "Nichate."

Matayo wadaima ni kumchata.

Yesu waatana Filipo ni Nasanaeli

Mawa lake, Yesu wadalamula kupita kumujhi wa Galilaya, kumeneko wadampheza Filipo, wadamkambila "Nichate."

Yao afunika kukhala oyaluzidwa a Yesu

Yapo adali mnjila, mundhu mmojhi wadamkambila Yesu, "Sinikuchateni kulikonjhe uko simupite." Yesu wadayangha, "Nghandwe zili ni mbhanga, ni mbalame za kumlengalenga zili ni visa, nambho mwana wa mundhu walibe pa malo pogona ni kupumulila."

Ndiipo, wadamkambila mundhu mwina, "Nichate." Nambho mundhu yujha wadayangha, "Ambuye, munisiye uti nipite nikaazike atate wanga." Nambho Yesu wadamkambila, "Asiye wandhu akufa waazike akufa anjao, nambho iwe pita ukaulalikile Ufumu wa Mnungu."

Mundhu mwina wadamkambila Yesu, "Ambuye, sinikuchateni, nambho munilole uti nipite nikalaile wandhu a kukhom langa." Yesu wadamkambila, "Palibe mundhu uyo wagwila khasu ni kuyamba kulima wapenyanjho mmbuyo, mundhu mmeneyo siwafunika kulowa mu Ufumu wa Mnungu."

O custo do discipulado

Seguir a Jesus exige renúncia. É preciso tomar a cruz diariamente, deixar tudo para trás e amar a Cristo acima de qualquer outro vínculo.

Ndiipo Yesu wadaakambila oyaluzidwa wake, "Mundhu uyo wafuna kunichata, poyamba wafunika wajhikane mwenewake ni kuutenga mtanda wake, wanichate.

"Ngati mundhu waliyonjhe wafuna kukhala woyaluzidwa wanga, ifunika wanikonde ine kupitilila umo waakondela atate wake na amake, mkazake ni wana, achakulu wake ni achalongo wake, ata kupitilila umo wajhikondela mwene wake. Ngati siwachita chimwecho, siwangakhoze kukhala woyaluzidwa wanga. Mundhu waliyonjhe uyo siwavemela kuvutika ni kumwalila yapo wanichata, siwakhoza kukhala woyaluzidwa wanga.

Petulo wadamkambila, "Ife tasiya kilakandhu takuchata iwe." Yesu wadakamba, "Zenedi nikukambiulani, kila mundhu uyo waisiya wandhu amnyumba yake, kapina mbale wake, kapina mlongo wake, kapina maye wake, kapina atate wake, kapina wana wake kapina minda yake ndande yaine ni ndande ya Uthenga Wabwino, siwalandile vindhu vochuluka pa ndhawi ya saino. Siwalandile nyumba, abale, alongo, maye, wana ni minda ni mavuto, ni masiku yayo yakujha siwalandile umoyo wa muyaya. Nambho, yawo achogolela siakhale kumbuyo, ni akumbuyo siachogolele."

Caminhar com Cristo

Quem segue a Jesus não anda em trevas, mas tem a luz da vida. Ele nos convida a crescer nele e a servir como Ele serviu.

Yesu ni dangalila la wandhu ajhiko

Ndiipo Yesu wadaakambilanjho, "Ine nde dangalila la jhiko la panjhi. Uyo wanichata siwaenda mu mdima, nambho siwakhale ni dangalila la umoyo."

Uyo wafuna kunitumikila lazima wanichate, ni paliponjhe yapo nili ine nde yapo sakhale ni atumiki wanga. Mundhu waliyonjhe uyo wanitumikila, Atate wanga sampache ulemu."

Nambho ngati tikauchota uzene kwa mtima wa chikondi sitikule chizimu ni sitimfikile Kilisito pa vindhu vonjhe, iye nde mlamuli wathu.

Seja o primeiro