Pular para o conteúdo
Publicidade

Vícios

Por Bíblia Online

A Bíblia nos alerta contra os vícios e comportamentos destrutivos. Deus nos chama à liberdade em Cristo, não à escravidão de desejos e hábitos que consomem corpo e alma.

A escravidão do pecado

Todo vício é uma forma de escravidão. Jesus veio para libertar os cativos e restaurar a verdadeira liberdade dos filhos de Deus.

Yesu wadayangha, "Uzene nikukambilani, uyo wachita machimo ni kapolo wa machimo.

Mwana wakakuchitani mlekeleledwe simulekeleledwe zenezene.

Mwana wakakuchitani mlekeleledwe simulekeleledwe zenezene.

Uzene siukulekeleleni

Ndiipo, Yesu wadaakambila Ayahudi yawo adamkhulupilila, "Mkayagwila mayaluzo yanga simukhale oyaluzidwa wanga azene. Simuujhiwe uzene, ni uzene siukulekeleleni."

Muusunge ufulu wanu

Kilisito wadatipacha ife ufulu, iye wadafuna tikhale afulu, chipano imani nganga simdavomela kukhalanjho pajhi pa ukapolo.

Mjhiwa kuti anyiiwe mkajhichocha mwachina wene ngati akapolo wa mundhu waliyonjhe mkhala akapolo azene amundhu yujha, ni ngati mkachichocha kukhla akapolo wa machimo mathelo yake ni nyifa, nambho mkachichocha kumvela Mnungu simkhale ovemelezeka kwa Mnungu?

Resistência e domínio próprio

O fruto do Espírito inclui o domínio próprio. O cristão é chamado a ter controle sobre seus desejos, resistir à tentação e vigiar contra as obras da carne.

kosakondwela mwina wakakhala ni chindhu, kulojhela mowa kudya kupunda ni vindhu vili ngati vimenevo. Nikuonyani ngati umo nidakuonyelani mmayambo, wandhu achita yameneyo saupata ufumu wa Amnungu.

wojhichicha ni kujhilamula umwene. Palibe thauko ilo lichogoza kuvichucha vindhu vimenevo.

Tumilani Mathupi yanu kwa ulemelelo wa Mnungu

Mundhu siwakhoze kukamba, "Navomelezedwa kuchita chindhu chilichonjhe." Yetu, nambho osati kila vindhu vali vabwino kwaiwe. Nikhoza kukamba navomelezedwa kuchita chindhu chilichonjhe, nambho sinifuna kulamulidwa ni chindhu chalichonjhe.

Tumilani Mathupi yanu kwa ulemelelo wa Mnungu

Mundhu siwakhoze kukamba, "Navomelezedwa kuchita chindhu chilichonjhe." Yetu, nambho osati kila vindhu vali vabwino kwaiwe. Nikhoza kukamba navomelezedwa kuchita chindhu chilichonjhe, nambho sinifuna kulamulidwa ni chindhu chalichonjhe.

Chimwecho, nilivuticha thupi langa ni kujhichekeleza kuti lichite ichonichifuna ni nikatho alalikila wina sinidakanidwa.

Mayeso yonjhe mwapata yakawaida kwa wandhu. Nambho Mnungu ni wokhulupilika siwavomela muyesedwe kupitilila yayo muyakhoza, nambho yapo muyesedwa, siwakupacheni njila yotulukila ili mukhoze kulimba mtima.

Mayeso yonjhe mwapata yakawaida kwa wandhu. Nambho Mnungu ni wokhulupilika siwavomela muyesedwe kupitilila yayo muyakhoza, nambho yapo muyesedwa, siwakupacheni njila yotulukila ili mukhoze kulimba mtima.

Chezelani ni kupembhela kuti msadalowa mu mayeselo. Mtima ufuna kuchita yayo yafunika, nambho thupi lilibe mbhavu."

Libertação e renovação

Em Cristo somos libertos de toda forma de dependência. Pela renovação da mente, aprendemos a discernir e rejeitar o que nos prende.

Ukhalo wa kumtumikila Mnungu

Chipano, achabale wanga, pakuti Mnungu ni walisungu kupunda, nikupembhani kwa mtima wanga wonjhe, mjhichoche mwachinawene kwa Amnungu mkhale ngati njhembe yo pyeleza iyo ili yamoyo, iyo ili ya Mnungu mwene ni yomkwadilicha Mnungu. Iyi nde njila yanu ya zene yakumlambila Mnungu. Simudaganizila ngati wandhu ajhiko lino umo aganizila, nambho Mnungu siwakung’anamuleni maganizo yanu kwa kuganizila bwino. Pamenepo ndipo simkhoze kujhiwa icho wafuna Mnungu ni kujhiwa chindhu chili cha bwino, ilo limkwadilicha ni kuchita ngati umo ifunikila.

Chinchijha anyiimwe ifunika mjhione kuti mwafa kwa nghani ya machimo, nambho ngati mkhala kwa umojhi ni Mnungu kwa kumkhulupilila Yesu Kilisito.

Chipano machimo siyadalamulanjho wiwalo va matupi yanu yayo siyafe, ni siyadakuchitani muyavele makumbilo yanu. Msidachichita chiwalo chilichonjhe cha matupi yanu kuhala chindhu cho chitila machimo. Pambuyo pake jhichocheni mwachinawenewake kwa Mnungu ngati wandhu mwa hyuka, vichocheni viwalo vanu kwa Mnungu ngati vindhu ivo vavomelezeka.

Pakuti ife talunjana niiye kwa njila nyifa yake, chimwecho ife sitilunjane naye kwa kuhyukichidwa ngati iye. Tijhiwa kuti vichito vathu va kale vidafa ni vidapachikidwa pa mtanda pamojhi niiye, kuti mbhavu za machimo ziwanangidwe, ni sitidakhalanjho akapolo a machimo.

O corpo como templo

Nosso corpo é templo do Espírito Santo. Devemos honrar a Deus com o corpo, fugindo da embriaguez, da imoralidade e de toda impureza.

Simujhiwa kuti mathupi yanu ni nyumba ya Mzimu Wamnungu, uwo ukhala mkati mwanu ni uwo mwapachidwa ni Mnungu? Mathupi yanu osati yanu mwachinawene nambho ni ya Mnungu,

Zene mujhiwa kuti anyiyawo achita voipa siapata ufumu wa Mnungu. Simdanyengeka Achigololo, kapina alambila viboliboli kapina akomana chithupi kumbuyo kwa maumbidwe, kapina anghungu, kapina akhumbila kuipa, kapina alojhela, kapina otukwana, kapina alanda anyiyawa siaupata Ufumu wa Mnungu. Akumojhi wanu adali amtundu umeneo. Nambho mudachukidwa ni mdakhala bwino kwa kuchochedwa machimo ni Mnungu, mwavomelezeka ni Mnungu kwa Ambuye Yesu Kilisito ni kwa Mzimu wa a Mnungu wathu.

Msiye kulojhela mowa, imeneyo siikutaizeni, nambho mchoghozedwe ni Mzimu wa Mnungu.

Mchele wa chinyope ni dangalila

"Anyiimwe ni mchele wa chinyope wa jhiko. Nambho mchele wa chinyopeo ngati wasukuluka sikomelechedwe ni chiyani? Ulibe njhito. Siutaidwe kubwalo nikupondedwa ni wandhu."

Msatiika mmayeso,

nambho utikengelele ni yujha Woipa.

Pakuti masiku yonjhe Ukulu ni wanu ni mbhavu ni ulemelelo mbaka muyaya. Amina."

Pakuti yalembedwa mmalembo ya Mnungu kuti,

"Ngati umo nikhalila Ambuye akamba,

Kila mundhu siwanigwadile,

kila mmojhi siwakambe mwene kuti ine ni Mnungu"

Chipano kila mmojhi wathu siwakambe nghani zake mwene pachogholo pa Mnungu.

Seja o primeiro