1 Abale wanga, yapo nidali kwanu sinidakhoze kukuyaluzani anyiimwe ngati umo nayaluzila wandhu ali ni mzimu wa Mnungu, nidafunika kukuyaluzani nianyimwe ngati wandhu muli ajhiko lino, mdali ngati wana waang'ono yawo simdakhoze kujhiwa bwino chikhulupi cha Kikilisito. 2 Nidakuyaluzani vindhu vopepuka ngati mujha maye wammwecha mwana wake likama, osati chakudya cholimba, nidachita chimwechi ndande simudali tayali kwachakudya cholimba. Ni ata chipano simuli tayali, 3 ndande muyendekela kukhala ngati umo wandhu ajhiko lino akhalila. Ngati muli ni njhanje pakati panu ni muli ni ndewo ni mwina, ili lichimikiza kuti muli ajhiko lino, bwanji mukhala bwino? 4 Akumojhi wanu akamba, "Timchata Poolo," ni wina, "Timchata Apolo" bwanji anyiimwe namwe muchita ngati wandhu ajhiko?
5 Bwanji, Apolo ni yani? Ni Poolo ni yani? Ife niatumikipe anyiyao a Mnungu adatitumila dala mumkhulupilile Yesu Kilisito. Kila mmojhi wathu wadachita njhito iyo wapachidwa ni Mbuye. 6 Ine nidavyala mbeu, Apolo wadamwazilila majhi, nambho Mnungu nde uyo wadachita ikule. 7 Chimwecho uyo wavyala mbeu ni uyo wamwazilila majhi sio kandhu. Nambho Mnungu yokha nde wamate uyo waichita ikule. 8 Palibe kusiyana pakati pa yujha wavyala ni wamwazilila majhi, Mnungu siwampache kila mundhu mbhaso yake kuchokana ni njhito iyo wachita. 9 Pakuti ife tichita njhito ya Mnungu pamojhi, ni anyiimwe nimunda wa Mnungu.
Anyiimwe ni nyumba ya Mnungu. 10 Kwa tandizo la ubwino wa Mnungu wanipacha ine, kukhala woyamba kukulalikilani anyiimwe uthenga wa Mnungu, ngati mujha fundi wakhoza kumanga nyumba yapo wayamba kumanga nyumba, ni mafundi wina akujha kumanga pamwamba pake. Nambo kila mmojhi wanu wakhale maso umo wamangila pamwamba pake. 11 Palibe mundhu mwina wapeleka mayaluzo yina pakuti mayaluzo yameneyo tayali yalipo nde Yesu Kilisito. 12 Oyaluza yawo ayaluza bwino mayaluzo ya Yesu yali ngati omanga yao amanga nyumba kwa kutumila zahabu, madini, ni myala ya mtengo wa ukulu nambho oyaluza yawo sayaluza bwino ali ngati omanga yawo amanga atumila mitengo, machamba au maujhu. 13 Pakuti siku limenelo kila njhito ya wandhu sidajhiwike umo ili, siku limenelo silijhe ni moto ni moto umenewo siupime kila njhito, ni moto siudaiyese njhito ni kuilangiza mtundu wake. 14 Ikakhala njhito ya mundhu ngati siiyomwa pamoto, siwalandile mbhaso. 15 Nambho ngati njhito ya mundhu siiyomwe pamoto, siwapata mbhaso, nambho iye mwene siwalamichidwe ngati mujha wachelembuka pa moto.
16 Zene mjhiwa kuti anyimwe ni nyumba ya Mnungu ni kuti Mzimu wa Mnungu ukhala mkati mwanu? 17 Mnungu siwamuwanange waliyonjhe uyo wawananga nyumba ya Mnungu, pakuti nyumba ya Mnungu ni yoyela kupunda, ni nyumba imeneyo nimwachina wene.
18 Msadajhinamiza, ngati mwina wanu wakajhiganiza waima pa jhiko, wafunika wakhale owowela kuti wapate kukhala ni hekima. 19 Hekima ya wandhu a jhiko lino ni usabwabwa pachogolo pa Mnungu, ngati umo malembo Mnungu yalembedwa, "Mnungu wakodwecha ahekima pakuchenjela kwao," 20 Yalembedwa chimwechi mmalembo yina, "Mbuye wajhiwa maganizo ya ahekima asati ya bwino." 21 Chimwecho mundhu wasajhidamila ivo wandhu avichita, ndande vindhu vonjhe vanu. 22 Poolo, Apolo, ni Petulo, jhiko lino, umoyo kapina nyifa, vindhu vachipano ni vapambuyo, ivi vonjhe ni vanu, 23 ni anyiimwe ni wandhu wake Kilisito, ni Kilisito ni wa Mnungu.