1 Achabale, paja nidajha kwanu, sinidajhe kukulalikilani Uthenga wa Mnungu kwa kukwanila, kapina kwa hekima ya wandhu. 2 Pajha nidali namwe, nidachita maganizo yanga yaiwalile kila kandhu ila Yesu Kilisito yokha ni nyifa yake pa mtanda. 3 Pajha nidajha kwanu, nidali ofooka ni wamandha ni kutendhemela kupunda, 4 ni mayaluzo yanga ni uthenga wanga siudali wa mau ya kwa kwadilicha wandhu, nambho kwa mbhavu ya Mzimu wa Mnungu. 5 Dala chikhulupi chanu chisakhala mu hekima ya wandhu nambho mu mbhavu za Mnungu.
6 Nambho tidakamba kwa hekima kwa wandhu akwanila mumzimu wa Mnungu, nambho osati hekima ya jhiko lino, kapina ya anyiyao alamula jhiko lino, anyiyao ulamulilo uli mgulu lotayika. 7 Hekima iyo niuzila ni uthenga wa uzene wa Mnungu ijha idabisika kwa wandhu mbaka saazino, iyi Mnungu wadaisangha kwa ulemelelo wathu kuyambila mmayambo. 8 Palibe mlamuli wa jhiko lino waijhiwa hekima iyi. Ngati adakaijhiwa, saadakapachika pamtanda Ambuye aulemelelo. 9 Atangati malembo ya Mnungu yalembedwa,
"Chijha mundhu siwadachione kapina mundhu kuchivela,
vindhu ivo mundhu siwadaviganizilepo kuti vichokele,
ivi nde ivo Mnungu wakonjela onjhe amkonda iye."
10 Nambho Mnungu watilangiza kupitila Mzimu wake. Mzimu upenyecha kila chindhu, ata vachisisi vamkati mwa Mnungu. 11 Palibe mundhu uyo wajhiwa maganizo ya mundhu mwina. Chimchijha mzimu wokha ulimkati nde ujhiwa maganizo ya mundhu mmeneyo, chimwecho ndeumo ili ata kwa Mnungu, Mzimu wokha wa Mnungu nde ujhiwa maganizo ya Mnungu. 12 Sitidalandile Mzimu wa jhiko nambho ife talandila Mzimu ujha wachokela kwa Mnungu, chimwecho sitijhiwe vonjhe ivo Mnungu watipacha ife.
13 Chimwecho sitikamba kwa mau ayaluza ali ni hekima, nambho mau wa yaluza Mzimu wa Mnungu, tikambilila vindhu va Uzimu kwa onjhe ali ni Mzimu wa Mnungu. 14 Uyo walibe Mzimu wa Mnungu siwakhoza kulandila mbhaso ikujha kuchokela kwa Mzimu wa Mnungu. Mundhu mmeneyo siwakhoza kuva yameneyo, waona kuti vindhu vimenevo vilibe mate, ndande yake yavunukulidwa muchizimu. 15 Uyo wali ni Mzimu wa Mnungu, wakhoza kulamula ngati umo ifunika, nambho siwakhoza kulamulidwa ni wandhu wina. 16 Ngati umo yalembedwa mmalembo ya Mnungu,
"Yani wajhiwa maganizo ya Mbuye?
Yani wakhoza kumkambila Mnungu chindhu chochita?"
Nambho ife tili ni maganizo ngati Kilisito.