Publicidade

1 Coríntios 10

Msadalambila viboliboli

1 Achabale, nifuna mujhiwe icho chidaachokela anya mbuye yao amamchata Musa. Adali panjhi pa mtambo, nionjhe adayomboka nyanja ya mchele ya shamu. 2 Adabatizidwa onjhe kwa mtambo ni kwa nyanja ya mchele ngati ochatila a Musa. 3 Wonjhe adadya chakudya chinchijha icho chidachokela kumwamba kwa Mnungu, 4 ni wonjhe adamwa chakumwa chinchijha chidacho kwa Mnungu. Adamwa kuchoka mujha mumwala waukulu wa uzimu uwo udachata, ni mwala waukulu umeneo udali Kilisito mwene wake. 5 Nambho wandhu ambili sadachite vindhu ivo Mnungu wadafuna, chimwecho adamwalila ni vitanda vao vidayenela kunghalambo.

6 Chipano vindhu ivi ni chifani kwathu, dala kutuonya tisidakhumbila voipa ngati umo adachitila anyiiwo, 7 msada lambila viboliboli, ngati umo adachita akumojhi wao. Ngati umo yalembedwa malembo ya Mnungu, "Wandhu adakhala ni kumwa niadaima kuvina magule ya wandhu osamjhiwe Mnungu." 8 Tisida chita chigololo ngati mujha adachitila akumojhi wao adagwa ni kumwalila wandhu elufu ishilini ni tatu. 9 Wala tisaayesa Ambuye ngati mujha adachitila akumojhi wao adamwalila kwa kulumidwa ni njoka. 10 Msidadandaulila yajha Mnungu wayachita ngati mujha adachitila akumojhi wao, Mnungu wadamtuma Mtumiki wa Mnungu wa kumwamba uyo wakupha kwaapha.

11 Basi vindhu ivi vidaapata anyiiwo ngati chifani kwatu, yadalembedwa dala kutionya ife. Tili amoyo pafupi ni mathelo ya jhiko.

12 Yujha waganiza kuti waima pachikhulupi wapenye siwadagwa ni kuchita machimo. 13 Mayeso yonjhe mwapata yakawaida kwa wandhu. Nambho Mnungu ni wokhulupilika siwavomela muyesedwe kupitilila yayo muyakhoza, nambho yapo muyesedwa, siwakupacheni njila yotulukila ili mukhoze kulimba mtima.

14 Chimwecho achabale wanga, thawani, msadalambila viboliboli. 15 Nikamba ni anyiimwe wandhu muli ni njelu, lamulani mwachinawene kwa nghani ya ivi nivikamba. 16 Chikho chijha cha mwawi tichitumila kwa chakudya cha Mbuye, sitigwilizana ni mwazi wa Kilisito? Ni yapo tibandhula lijha bumunda, sitigwilizana ni thupi la Kilisito? 17 Pakuti bumunda nilimojhi, ife taonjhe tili ambili tili thupi limojhi, taonjhe tililandila bumunda limwelo limojhi.

18 Apenyeni wandhu a Izilaeli, anyiwajha wonjhe akudya chakudya chamahoka alunjana ni mazabao imeneyo. 19 Chipano, nikambe chiyani, kuti chijha chachochedwa njhembe kwa viboliboli ni chindhu? 20 Osati! Nambho ichonikamba nikuti, njhembe izo achocha wandhu siamjhiwa Mnungu. Simwachochela Amnungu nambho muvichochela viwanda, nane sinifuna anyiimwe mkhale ni mgwilizano ni viwanda. 21 Simukhoza kukhala pa pwando la Ambuye pamojhi ni viwanda. Simukhoza kudya chakudya ni kumwa pamojhi pa pwando la Ambuye ni kugwilizana kudya chakudya ni kumwa pamojhi pa pwando la viwanda. 22 Bwanji, tifuna kwachita Ambuye akhale ni njhanje? Mganiza tili ni mbhavu kupitilila iye?

23 Wandhu wina akamba "Vindhu vonjhe valoledwa, yetu, nambho ine nikamba asati kila chindhu ni chabwino," Chimwecho wina akamba, "Vindhu vonjhe valoledwa nambho asati kila chindhu chifunika." Nambho ine nikamba osati kila chindhu chitangatila kulilimbicha gulu la wandhu akhulupilila Kilisito. 24 Mundhu, waliyonjhe siwada funafuna vindhu vake mwene nambho wafunefune ni vindhu va wina.

25 Muvomeledwa kudya kila icho chigulichidwa pamalo pa malonda wandhu ambili, popande kufunjha funjha kujhiwa ngati chabwino kapina opande chabwino kudya. 26 Kwaife, yalembedwa mu malembo ya Mnungu, "Jhiko ni vindhu vonjhe ivo vilimo ni chuma cha Mbuye."

27 Mundhu uyo siwadakhulupile wakakulalika kuchakudya, ni namwe mufuna kupita, idyani kila chindhu icho simuikilidwe popande kufunjha mafunjho yaliyonjhe ngati chabwino kapina osati chabwino. 28 Nambho mundhu wakakukambila, "Nyama iyi ya chochedwa njhembe kwa viboliboli," msadya ndande ya kumuyaluza iye dala simudapwetekedwa mmitima yanu. 29 Yapa nikamba osati ndande ya kupweteka maganizo yanu nambho nikamba ndande ya kupweteka maganizo ya iye wakupacha.

Simunifujhe, "Ndande yanji yajha nifuna kuchita ine yalamulidwe ni maganizo ya mundhu mwina? 30 Ngati ni muyamika Mnungu kwa chakudya changa, ndande yanji nilamulidwe kwa chakudya ichi nimuyamika Mnungu?"

31 Chimwecho, chalichonjhe icho mchita, ikakhala mkudya kapina kumwa, chitani yonjhe kwa kumtamanda Mnungu. 32 Mjhikala chimwecho, msadachiticha Ayahudi kapina Agiliki kusiya kumkhulupilila Kilisito kapina msadalichita gulu la wandhu wa Mnungu kuchita machimo. 33 Mchite ngati umo ine nichitila, nayesa kwakwadilicha kwamujha nachitila, pakuti sinifunafuna vabwino ndande yanga namwene, nambho nifunafuna vabwino ivo sivathangatile wina dala akhoze kuomboledwa.

Veja também

Publicidade
1 Coríntios
Ver todos os capítulos de 1 Coríntios
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-19_11-20-24-