Publicidade

Gálatas 5

Muusunge ufulu wanu

1 Kilisito wadatipacha ife ufulu, iye wadafuna tikhale afulu, chipano imani nganga simdavomela kukhalanjho pajhi pa ukapolo. 2 Vechelani! Ine ni Poolo nikamba namwe! Ngati mkavomela kuchitidwa mdulidwe ndande ya kuvela thauko la Musa, Kilisito walibe mate yaliyonjhe muukhalo wanu. 3 Nikambanjho padanga, waliyonjhe uyo wavomela kuchitidwa mdulidwe wafunika waligwile thauko lonjhe. 4 Ngati mkapenyelela kuchitidwa wovemelezeka kwa kupitila kugwila thauko, pamenepo simkale mwajhiika kutali ni Kilisito, mwausiya ubwino wa Mnungu. 5 Pakuti ife tilindilila kwa chikhulupilila ni kwambhavu ya Mzimu, tichitidwe wovomelezeka kwa njila ya kumkhulupilila Kilisito. 6 Pakuti Ikakhala talunjhana ni Kilisito Yesu, kuchitidwa mdulidwe kapina kosachitidwe mdulindwe kulibe mate, cha mate kuhichita njhito kwa chikondi nde uko kulangiza kukhulupilila kwathu.

7 Mmayendekela bwino! Yani basi, wakuchekelezani simdauvela uzene? 8 Mnungu uyo wakutanani siwadakuchiticheni mchite chimwecho. 9 Unami pang'ono uwananga mayaluzo yonjhe ya uzene! 10 Kuchokana ni kulunjana kwatu ni Ambuye, nikukhulupilila kupunda anyiimwe kuti mdali pamojhi ni ine, ni waliyonjhe uyo wakuchauchani siwalangidwe.

11 Achaabale wanga ngati ine nikali niyendekela kwalalikila wandhu kuchitidwa mdulidwe kwa kuchata thauko la Musa, ndande yanji chipano nivutichidwa ni Ayahudi? Ngati nimakalalikila chimwecho, kulalikila kwanga nghani za nyifa ya Yesu Kilisito pamtanda sikudakaipicha Ayahudi. 12 Nibwino wandhu amenewo akuchauchani paghani za kuchitidwa mduludwe adakayadula maumbidwe yawo achinawene. 13 Pakuti anyiimwe mdatanidwa ni Mnungu dala mkale afulu, ufulu wanu usidakhala ndande yochata makumbilo ya thupi, nambho mfunika mtumikilane kwa chikondi. 14 Pakuti thauko lonjhe likwanilichidwa kwa lamulo lino limojhi, "mkonde wa pafupi wako ngati umo ujhikondela wamwene." 15 Ngati mkalumana ni kutafunana ngati zinyama, mjhipenyelele msayomwechana anyiimwe kwa anyiimwe!

Kuchogozedwa ni Mzimu wa Mnungu

16 Chipano nikamba chimwechi, ukhalo wanu uchogozedwe ni Mzimu wa Mnungu, mkachita chimwecho simuchatanjho makumbilo yoipa. 17 Pakuti makhumbolo yoipa yachuchana ni makhumbilo ya Mzimu wa Mnungu, nayo Mzimu wa Mnungu siwakhumbila vindhu voipa. Vindhu vimenevo vichuchana, ndande imeneyo simkhoza kuchita yayo mfuna. 18 Ngati mkachogozedwa ni Mzimu wa Mnungu, basi simuchogozedwa ni thauko la Musa.

19 Vichito va jhiko vijhiwika navo nde ivi, uhule, chigololo, ni ukhalo woyipa, 20 kulambila viboliboli, ufiti, udani, ndewo, njhanje, mbwayi, chipili, mkangano ni kosavana, 21 kosakondwela mwina wakakhala ni chindhu, kulojhela mowa kudya kupunda ni vindhu vili ngati vimenevo. Nikuonyani ngati umo nidakuonyelani mmayambo, wandhu achita yameneyo saupata ufumu wa Amnungu.

22 Nambho ivo vichokela ukachogozedwa ni Mzimu wa Mnungu ni chikondi, kukondwela, mtendele, kulimba mtima, ubwino, kutangatila wina ni kukhulupilika, 23 wojhichicha ni kujhilamula umwene. Palibe thauko ilo lichogoza kuvichucha vindhu vimenevo. 24 Anyiwajha ali ni Kilisito aupachika pamtanda ukhalo wao wa chijhiko pamojhi ni maganizo yake yoipa ni makumbilo yake. 25 Tikakhala kwa mthandizo wa Mzimu wa Mnungu, ifunika chinchijha tichate uchogolelo wake. 26 Basi sitidajhidama, sitadayambana kapina kuonelena njhanje.

Veja também

Publicidade
Gálatas
Ver todos os capítulos de Gálatas
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-18_14-04-22-