Pular para o conteúdo
Publicidade

Resultados da busca por "salvação"

75 resultados encontrados

  1. Isaías 38

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 38
    Mostrando versículos 7–20 de 22

    7" ‘Ichi ndi chizindikiro cha Yehova kwa iwe kutsimikiza kuti Yehova adzachita zimene walonjeza:

    16Ambuye, masiku anga ali mʼmanja mwanu.Mzimu wanga upeza moyo mwa Inu.Munandichiritsa ndikundikhalitsa ndi moyo.

    20Yehova watipulumutsa.Tiyeni tiyimbe ndi zoyimbira za zingwemasiku onse a moyo wathumʼNyumba ya Yehova.

  2. 1 Crônicas 11

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 11
    Mostrando versículos 27–40 de 47

    27Samoti Mharori,Helezi Mpeloni.

    32Hurai wa ku zigwa za Gaasi,Abieli Mwaribati,

    40Ira Mwitiri,Garebu Mwitiri,

  3. Salmos 76

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 76
    Mostrando versículos 2–9 de 12

    2Tenti yake ili mu Salemu,malo ake okhalamo mu Ziyoni.

    7Inu nokha ndiye muyenera kuopedwa.Angathe kuyima pamaso panu ndani mukakwiya?

    9pamene Inu Mulungu munadzuka kuti muweruze,kupulumutsa onse osautsidwa mʼdziko.Sela

  4. Tito 2

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 2
    Mostrando versículos 9–13 de 15

    9Phunzitsa akapolo kuti azigonjera ambuye awo mu zinthu zonse ndi kuwakondweretsa. Asamatsutsane nawo

    11Pakuti chisomo cha Mulungu chimene chimapulumutsa chaonekera kwa anthu onse.

    13pamene tikudikira chiyembekezo chodala; kuonekera kwa ulemerero wa Mulungu wathu wamkulu ndi Mpulumutsi, Yesu Khristu,

  5. Atos 11

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 11
    Mostrando versículos 14–26 de 30

    14Iye adzakuwuza uthenga umene udzapulumutsa iwe ndi a pa banja ako.’

    25Kenaka Barnaba anapita ku Tarisisi kukafuna Saulo,

    26ndipo pamene anamupeza anabwera naye ku Antiokeya. Barnaba ndi Saulo anasonkhana ndi mpingo kwa chaka chimodzi naphunzitsa anthu ambirimbiri. Okhulupirirawo anayamba kutchedwa Akhristu ku Antiokeya.

  6. Êxodo 35

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 35
    Mostrando versículos 2–14 de 35

    2Muzigwira ntchito zanu pa masiku asanu ndi limodzi, koma tsiku la chisanu ndi chiwiri likhale la Sabata, tsiku lanu lopuma, lopatulika kwa Yehova. Aliyense amene adzagwira ntchito iliyonse pa tsikuli ayenera kuphedwa.

    6nsalu zobiriwira, zapepo, zofiira, nsalu zofewa; ubweya wambuzi;

    14choyikapo nyale yowunikira pamodzi ndi zipangizo zake, nyale ndi mafuta anyalezo;

  7. 1 Samuel 10

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 10
    Mostrando versículos 1–27 de 27

    1Ndipo Samueli anatenga botolo la mafuta nathira mafutawo pa mutu wa Sauli ndipo anapsompsona nati, "Yehova wakudzoza kuti ukhale mtsogoleri wa anthu ake, Aisraeli. Iwe udzalamulira anthu a Yehova ndiponso udzawapulumutsa mʼmanja mwa adani awo owazungulira. Chizindikiro chakuti Yehova wakudzoza kuti ukhale mtsogoleri wa anthu ake ndi ichi:

    13Sauli atasiya kuloserako, anapita ku kachisi ku phiri.

    27Koma anthu ena achabechabe anati, "Kodi munthu uyu angathe bwanji kutipulumutsa?" Iwo anayamba kumunyoza Sauliyo, ndipo sankamupatsa ngakhale mphatso. Koma iye sanalabadireko.

  8. Hebreus 6

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 6
    Mostrando versículos 2–18 de 20

    2za maubatizo, za kusanjika manja, za kuuka kwa akufa ndi za chiweruzo chotsiriza.

    5Analawa kukoma kwa mawu a Mulungu ndi mphamvu za nthawi ikubwera.

    18Mulungu anachita zinthu ziwiri, lonjezo ndi lumbiro, zimene sizingathe kusintha ndipo Mulungu sangathe kunama. Choncho Mulungu akutilimbikitsa mtima ife amene tinathawira kwa Iye kuti tichigwiritsitse chiyembekezo chimene tinalandira.

  9. Levítico 16

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 16
    Mostrando versículos 25–31 de 34

    25Mafuta a nyama yopepesera machimo awatenthe pa guwa lansembe.

    28Munthu amene azitenthe achape zovala zake ndi kusamba. Pambuyo pake alowe mu msasa.

    31Limeneli ndi tsiku lanu la Sabata lopumula, ndipo muzigonja pamaso pa Yehova. Limeneli ndi lamulo lanu la muyaya.

  10. Gênesis 37

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 37
    Mostrando versículos 15–22 de 36

    15munthu wina anamupeza akungozungulirazungulira mʼmunda ndipo anamufunsa, "Ukufunafuna chiyani?"

    21Koma Rubeni atamva izi, anapulumutsa Yosefe. Iye anati kwa abale ake, "Ayi, tisamuphe,

    22tisakhetse magazi. Tiyeni timuponye mʼchitsime ku chipululu konkuno. Koma tisamuvulaze nʼkomwe. Rubeni ananena zonsezi kuti apulumutse Yosefe ndi kuti pambuyo pake akamupereke kwa abambo awo."

  11. Gálatas 6

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 6
    Mostrando versículos 7–18 de 18

    7Musanamizidwe: nʼkosatheka kupusitsa Mulungu. Munthu amakolola zimene wafesa.

    9Tisatope nʼkuchita zabwino, pakuti pa nthawi yoyenera tidzakolola ngati sititopa.

    18Chisomo cha Ambuye athu Yesu Khristu zikhale ndi mzimu wanu abale. Ameni.

  12. Neemias 7

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 7
    Mostrando versículos 30–66 de 73

    30Anthu a ku Rama ndi Geba 621  

    48Zidzukulu za Lebana za Hagaba, ndi za Salimayi,  

    66Chiwerengero chonse cha anthuwa chinali 42,360.

  13. Lucas 24

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 24
    Mostrando versículos 2–51 de 53

    2Anaona mwala wa pa manda utagubuduzika

    47Ndipo kutembenuka mtima ndi kukhululukidwa kwa machimo zidzalalikidwa mu dzina lake kwa anthu amitundu yonse kuyambira mu Yerusalemu.

    51Iye akuwadalitsa, anawasiya ndipo anatengedwa kupita kumwamba.

  14. Jó 31

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 31
    Mostrando versículos 2–14 de 40

    2Kodi Mulungu kumwambako wandisungira zotani?Kodi cholowa changa chochokera kwa Wamphamvuzonse kumwambako nʼchotani?

    12Ndi moto umene umayaka mpaka chiwonongeko;ukanapsereza zokolola zanga.

    14ndidzatani pamene Mulungu adzanditsutsa?Nanga ndidzayankha chiyani akadzandifunsa?

  15. Salmos 18

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 18
    Mostrando versículos 2–46 de 50

    2Yehova ndiye thanthwe langa, chitetezo changa ndi mpulumutsi wanga;Mulungu wanga ndi thanthwe langa mʼmene ndimathawiramo.Chishango changa ndi ndodo yachipulumutso changa, ndi linga langa.

    19Iye anandipititsa kumalo otakasuka;anandipulumutsa chifukwa amakondwera nane.

    46Yehova ndi wamoyo! Litamandidwe Thanthwe langa!Akuzike Mulungu Mpulumutsi wanga!

  16. Números 7

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 7
    Mostrando versículos 46–82 de 89

    46mbuzi yayimuna imodzi ya nsembe yopepesera machimo;

    64mbuzi yayimuna imodzi ya nsembe yopepesera machimo;

    82mbuzi yayimuna imodzi ya nsembe yopepesera machimo;

  17. 1 Crônicas 14

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 14
    Mostrando versículos 4–7 de 17

    4Mayina a ana amene anaberekera ku Yerusalemu anali awa: Samua, Sobabu, Natani, Solomoni,

    5Ibihari, Elisua, Elipeleti,

    7Elisama, Beeliada ndi Elifeleti.

  18. Provérbios 29

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 29
    Mostrando versículos 5–25 de 27

    5Munthu woshashalika mnzake,akudziyalira ukonde mapazi ake.

    10Anthu okhetsa magazi amadana ndi munthu wangwirokoma anthu olungama amasamalira moyo wake.

    25Kuopa munthu kudzakhala ngati msampha,koma aliyense amene amadalira Yehova adzatetezedwa.

  19. Isaías 61

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 61
    Mostrando versículos 2–10 de 11

    2Wandituma kuti ndikalengeze nthawi imene Yehova adzapulumutsa anthu ake;za tsiku limene Yehova adzalanga adani a anthu ake.Wandituma kuti ndikatonthoze olira.

    3Wandituma kuti ndiwakonzere olira a ku Ziyoni,nkhata ya maluwa yokongolamʼmalo mwa phulusa,ndiwapatse mafuta achikondwereromʼmalo mwa kulira.Ndiwapatse chovala cha matamandomʼmalo mwa mtima wopsinjika.Ndipo iwo adzatchedwa mitengo ya thundu yamphamvu yachilungamo,yoyidzala Yehovakuti Iye mwini apezemo ulemerero wake.

    10Ine ndikusangalala kwambiri chifukwa cha Yehova;moyo wanga ukukondwera chifukwa cha Mulungu wanga.Pakuti Iye wandiveka zovala zachipulumutso,ndipo wandiveka mkanjo wachilungamo.Zili ngati mkwati wovala nkhata ya maluwa mʼkhosi mwake,ndiponso ngati mkwatibwi wovala mikanda yamtengowapatali.

  20. Lucas 12

    Tsekulani Mawu a Mulungu mu Chichewa Chalero
    Capítulo 12
    Mostrando versículos 23–25 de 59

    23Moyo uposa chakudya, ndi thupi liposa chovala.

    24Taonani makwangwala: iwo safesa kapena kukolola, alibe nyumba zosungamo zinthu kapena nkhokwe; komabe, Mulungu amawadyetsa. Koposa kotani inu amene ndi ofunikira kuposa mbalame.

    25Ndi ndani wa inu akhoza kuwonjeza ora pa moyo wake chifukwa cha kudandaula?

Léxico (correspondência exata) Semântico (correspondência relacionada) Versículos omitidos Contexto do capítulo