Publicidade

Resultados da busca por "amor"

24 resultados encontrados

4Mkwiyo umadzetsa nkhanza ndipo kupsa

5Kudzudzula munthu poyera nʼkwabwino

6Munthu amene amakukonda ngakhale akupweteke

4Mfumu imalimbitsa dziko poweruza mwachilungamo,

5Munthu woshashalika mnzake,

6Munthu woyipa amakodwa ndi machimo

3Ngati ndipereka zanga zonse kwa

4Chikondi nʼcholeza mtima, chikondi nʼchokoma mtima, chilibe nsanje, sichidzikuza, sichidzitamandira.

5Chikondi chilibe mwano, sichodzikonda, sichipsa mtima msanga, sichisunga mangawa.

4kapena kumangoyika mitima pa nthano

5Cholinga cha lamuloli ndi chikondi, chomwe chimachokera mu mtima woyera, chikumbumtima chabwino ndi chikhulupiriro choona.

6Anthu ena anapatuka pa zimenezi

13Pakati pa zamayozo panali chinthu

14Zamoyozo zinkathamanga uku ndi uko ngati kungʼanima kwa mphenzi.

15Pamene ndinali kuyangʼana zamoyozo, ndinangoona mikombero ndipo pansi pambali pa chamoyo chilichonse panali mkombero umodzi.

1Yamikani Yehova chifukwa ndi wabwino.

2Yamikani Mulungu wa milungu.

3Yamikani Ambuye wa ambuye,

13Kanaani anabereka mwana wake wachisamba

14Ayebusi, Aamori, Agirigasi

15Ahivi, Aariki, Asini

8Ngati ndi kulimbikitsa, musiyeni alimbikitse.

9Chikondi chikhale chopanda chinyengo. Dana nacho choyipa; gwiritsitsa chabwino.

10Mukondane kwathunthu monga abale. Lemekezanani wina ndi mnzake kuposa inu eni.

2Mutamandeni chifukwa cha machitidwe ake

3Mutamandeni poyimba malipenga,

4Mutamandeni ndi matambolini ndi kuvina,

7Chimaliziro cha zinthu zonse chili

8Koposa zonse muzikondana wina ndi mnzake kwambiri, chifukwa chikondi chimaphimba machimo ambiri.

9Muzisamalirana wina ndi mnzake osamanyinyirika.

15Kanaani anabereka mwana wake wachisamba,

16Ayebusi, Aamori, Agirigasi;

17Ahivi, Aariki, Asini,

6Ichi nʼchifukwa chakenso inu mumapereka

7Mubwezereni aliyense amene munamukongola. Ngati inu muli ndi ngongole yamsonkho, perekani msonkho kwa oyenera kuwalipira. Ngati ndi kuopa perekeni kwa oyenera kuwaopa ndipo ngati ndi ulemu kwa oyenera ulemu.

8Musakhale ndi ngongole ndi wina aliyense kupatula ngongole ya kukondana wina ndi mnzake. Pakuti amene amakonda munthu mnzake wakwaniritsa lamulo.

6Ife ndi ochokera kwa Mulungu,

7Anzanga okondedwa, tiyeni tikondane wina ndi mnzake, pakuti chikondi chimachokera kwa Mulungu. Aliyense amene ali ndi chikondi ndi mwana wa Mulungu ndipo amadziwa Mulungu.

8Aliyense amene alibe chikondi sadziwa

2Mchombo wako uli ngati chikho

3Mawere ako akuoneka ngati ana awiri a mbawala,

4Khosi lako lili see! ngati

5Pomenyedwa, kuponyedwa mʼndende ndi mʼzipolowe.

6pokhala moyo woyera mtima, pomvetsa zinthu, wokoma mtima ndi wachifundo mwa Mzimu Woyera ndi mwachikondi choonadi

7ndi poyankhula choonadi mwamphamvu ya

2"Kodi iwe Yobu utsiriza liti

3Chifukwa chiyani ukutiyesa ngati ngʼombe

4Iwe amene ukudzipweteka wekha ndi

1Pitirizani kukondana monga abale.

2Musayiwale kusamalira alendo, pakuti pochita

5Ndinanyamuka kukamutsekulira wachikondi wangayo,

6Ndinamutsekulira wachikondi wanga,

7Alonda anandipeza

13Khalani tcheru; khazikikani mʼchikhulupiriro chanu;

14Chitani zonse mwachikondi.

15Mukudziwa kuti a mʼbanja la

3kuchokera ku mtsinje wa Sihori

4Dziko lina la Akanaani ndi Ameara limene lili mʼmanja mwa Asidoni mpaka ku Afeki, dziko limene linachitana malire ndi dziko la Aamori.

5Palinso dziko lonse la Gebala

Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-20_17-16-08-