Pular para o conteúdo
Publicidade

NYIMBO YA SOLOMONI 2

10 Bwenzi langa anayankha ndipo anati kwa ine,

"Dzuka bwenzi langa,

wokongola wanga, ndipo tiye tizipita.

11 Ona, nyengo yozizira yatha;

mvula yatha ndipo yapitiratu.

Veja também