10 Bwenzi langa anayankha ndipo anati kwa ine,
"Dzuka bwenzi langa,
wokongola wanga, ndipo tiye tizipita.
11 Ona, nyengo yozizira yatha;
mvula yatha ndipo yapitiratu.
10 Bwenzi langa anayankha ndipo anati kwa ine,
"Dzuka bwenzi langa,
wokongola wanga, ndipo tiye tizipita.
11 Ona, nyengo yozizira yatha;
mvula yatha ndipo yapitiratu.