Publicidade

Gênesis 41

15 Farao anati kwa Yosefe, "Ndinalota maloto ndipo palibe amene watha kunditanthauzira. Tsono ndawuzidwa kuti iwe ukamva loto umadziwanso kulimasulira."

16 Yosefe anamuyankha Farao kuti, "Sindingathe koma Mulungu apereka yankho limene Farao akufuna."

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-29_22-07-56-