Publicidade

Jeremias 17

9 Mtima wa munthu ndi wonyenga kupambana zinthu zonse

ndipo kuyipa kwake nʼkosachizika.

Ndani angathe kuwumvetsa?

10 "Ine Yehova ndimafufuza mtima

ndi kuyesa maganizo,

ndimachitira munthu aliyense molingana ndi makhalidwe ake

ndiponso moyenera ntchito zake."

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-29_22-07-56-