9 Mtima wa munthu ndi wonyenga kupambana zinthu zonse
ndipo kuyipa kwake nʼkosachizika.
Ndani angathe kuwumvetsa?
10 "Ine Yehova ndimafufuza mtima
ndi kuyesa maganizo,
ndimachitira munthu aliyense molingana ndi makhalidwe ake
ndiponso moyenera ntchito zake."