Publicidade

Jeremias 31

9 Adzabwera akulira;

koma Ine ndikuwatonthoza mtima, ndidzawaperekeza.

Ndidzawatsogolera ku mitsinje yamadzi

mʼnjira yosalala mmene sadzapunthwamo.

Chifukwa ndine abambo ake a Israeli,

ndipo Efereimu ndi mwana wanga woyamba.

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-29_22-07-56-