Publicidade

Jeremias 5

14 Chifukwa chake Yehova Mulungu Wamphamvuzonse akuti,

"Popeza kuti anthu awa ayankhula mawu amenewa,

tsono mawu anga ndidzawasandutsa moto mʼkamwa mwako

ndipo anthu awa ndidzawasandutsa nkhuni zimene moto udzapserezeretu.

Veja também

Publicidade
Bíblia Online Bíblia Online

Bíblia Online • Versão: 2026-06-22_10-02-25-